Email a copy of 'Teacher wins in MCP primary elections in Mchinji West' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

7 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
opportunist
opportunist
7 years ago

Congrats

mwachande
mwachande
7 years ago

heeeheede iwe rodriguas ukuti chani iwe….akazi ako sanakuwuzebe zoona kuti nawonso anayamba kumwa uwafunse akumasule pepa ndaulula pepa

Kokota
Kokota
7 years ago

NGAKHALE INE SI SAPOTA WA MCP KOMA NDINAKAKHALA KU DELA LIMENELI PANO NDITAMUVOTERA MPHUNZITSI KWA INE NDI GREAT ACHIVEMENT NDITHU TIYENI TISAPANGE KADUKA DZIKO NDILATHU TIKAMUVOTERE NKULU AMENEYU ZIKOMO

Rodriguas
Rodriguas
7 years ago

Koma adapanga chibwenzi ndi mzimai odawala matendawa(akumwa) wapaboma pa Mchinji, wakashop mumsika. Ndiye kaya!
Komanso tamvetsedwa kuti boma likusintha date lamasankho mpaka september, 2016. Ndiye tindalama tonse titheratu tsiku lisadafike. Palinso chikonzero chakuti afinye kasalary kamkuluyu, salandiranso mpaka kale kuti campaign imvute. Nanga titi kuchipani kutuluka saka lomthandizira. Chifukwa malinga ndi mbiri, zimavuta kuthamdizapo. Kaya kapena.
Izi tangoti zidziwike kuopera pamawa nkudzati bwanji sim’datiuze. Dzimvere.

phinduka.
phinduka.
7 years ago

as a public officer,Dpp is going to fire him very soon becouse he is from opposition.

suspect zero37
7 years ago

komatu sikuti muziona ngati gwape ameneyi azawina ma by-election mwaalemba m’madzi

Jo
Jo
7 years ago

congrants Mr Mwale MCP motooooooo

Read previous post:
Malawian killed in South Africa mob attack: Three Malawians arrested

A 23-year-old Malawian man was  killed in a suspected mob justice attack in  Johannesburg, South Africa Sunday and police in...

Close