Email a copy of 'Thugs invade Fr Mulomole’s office at Zomba Diocese' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Thugs invade Fr Mulomole’s office at Zomba Diocese' to a friend
Ivory and rhino horns recently seized at Suvarnabhumi airport in Thailand were not from Malawi, the director in the Department...
oho
APA NDIYE PITALA WA GENDA KU POLICE CHAMBA CHILI MTHUMBA KKKKKKKK
AKATOLIKA??????? EEEEEEE KHALA PHEEE UFULU UMENE UKUDYELERAWU CHI CHIFUKWA CHA AMENEWA
NDIYE UKUTI APANGE CHIPANI CHAWO??? AKATOLIKAWO????? WATHADI MAPULANI KKKKKKKKKK
kunena kuti akatolika otchipa amavoyera dpp,ndiye mwalakwitsa.Kapena ndinu mwana simukudziwa zimene mcp yanuyo idatichita akatolikaffe mu 1992 after that first Pastoral letter,mufunse,which catholic are you talking about.
Everyone will vote for people that are similar to his/her character. Manyaka adzavotela manyaka amzake kkkkkkk
Munthu wa nzeru amamvetsera ena akamalankhula. Tamvetserani inu a dpp, akuliratu ndi eni ake adzikoli, musawatenge ngati zitsilu. Akukuuzani zoona inu mukutuma mbava ndi cholinga choti achite mantha asalankhulenso. So sad.
Malawians please if you really love your do not allow dpp to rule this country beyond 2019. This party and its leadership is known for all sorts of evil. Chakwera has to come in please!
Tikuonani 2019.
I was about to reply to a certain comment written by wakhunyu,koma basi ndasiya coz ndiwakhunyudi kapena kuti ndwe wa chifufu pa zomwe walembabzo.ndaona kuti akulimbana ndikutukwana CHAKWERA instead of kuti azilimbana ndi nkhumba yakeyi..anyway,ndakuvetsetsa poti ndiwe wakhunyudi.
Don’t listen to those wolves in sheep’s clothes .Atumidwa ndi mzao uja anathawa kutumikila ambuye.Whatever you say DPP will win come 2019 ngati anawina Ali kotsuta what more panopa. mulira misozi ya magazi.
Mwaba iba ndalama zamisonkho yathu pano mwati tikawalowere akatolika. Akupangileni novena ya 9day m’mapemphero ndikusala kudya mukhaule mugidwa nonse muona.