Email a copy of 'Toilet turned into a teacher’s house in Malawi' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

47 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
Luke Bukani
Luke Bukani
9 years ago

Zochitika Ku Mw.

Roma
9 years ago

Ndizomvetsa chisoni.Dele a kuedu. mukamava zimenezi chakudya chimalowa bwinobwino kukhosi kwanu,nkumasangalala?ntchito yanu ndikusokoneza aphunzitsi pa ntchito yawo?

GADABWALI
GADABWALI
9 years ago

The govt is full öf stupid ministers especialli minister of edu.

bakayawo
bakayawo
9 years ago

Koma sala ndiye kuphunzitsa ku town munakufunatu. Mpaka mthoyaz!

Munyapa pakhwili
9 years ago

Wamisala osagenda kkkkkkkkkkkk!!!!!!!!! Ndiye mukuti ndikamchimbuzi?

Munyapa pakhwili
9 years ago

Misala ilipo yamitundu mitundu mphuzitsiyu akufunika check up

zanga phee
zanga phee
9 years ago

Sikuti nyumba zikusowa, nkhani ndi yakuti amalandira ndalama yochepa , yoti sangakwanitse kulipira lendi ndi Transport kuphatikizapo zinthu zina zofunika pa moyo wamunthu chifukwa akanatha kukakhala kwa kachere, kubangwe , BCA, Ndirande , Machinjiri mix makhetha, chilobwe ndi kwina pongotchulapo madera ochepa, kodi chimbuzicho chinasiya kugwiritsidwa ntchito liti? chifukwa tikhoza kumangoti ndi chimbuzi chitasiya kugwira ntchito nthawi ya Kamuzu .

weddington kamanga
9 years ago

Kodi komweko kulibe school commitee?Kumadalila boma zilIzonse mapeto ake ndiwomwewo.

Luke C. G. Blueker
Luke C. G. Blueker
9 years ago

I feel sory 4 my nation. I think u leaders u r taking full advantage of us bcz we r poor. But knw that God sees us and will let us pass through these kinds of stituation.

Mkonda Amalawi
Mkonda Amalawi
9 years ago

Mbyofo mbyofo Pitala is wasting time sign some graffiti in Lumbadzi corner and painting filthy corner in police cells while teachers are sleeping toilets.All those allowances would have built a modest house for such a poor soul in such an unappreciated profession.Shame indeed.

Read previous post:
Malawi police shoot dead 2 carjacking suspects: Warning of graphic photo!

Malawi Police in Dedza Monday morning shot dead two armed robbers for trying to hijack a car and third suspect is battling...

Close