thy killed a person they need t killed also. They removed someone’s flesh remove theirs too
Vaanwyk ku Mzuzu
8 years ago
yemwe amamugulisayo afunsidwe bwino. mwina inali deal ndie wangowapachika anzakeo poti anadulisa mafupawo. munthu sangango bwela kwa ine kut ndimugule mango pomwe ine sindidya mangowo. no smoke without fire.
k.laston
8 years ago
anthu oipa awa alandile chilango chokhwima kuti wena atengelepo phunzilo chifukwa cha khalidwe loipali.kufuna kulemela mu njira yoipa ya chidule .kuchitabwino sathamangila ai anthu opepela lero dzawavuta.
iv
ankhoma
8 years ago
look at them. stupit.
lawrent malongo
8 years ago
It need to give them life in prison,anthuwa ndiwoipa osamawanyengelera.zilango zikumakhala zophweka ndichifukwa chake sakuleka moyo oipawu.
chidumayo
8 years ago
Last time a group of human bones sellers from Mozambique were given a bell of k20,000.00. This indicates that its not a serious offence. Can we revisit our laws. Shitiiiiiiiiiiiiiii Nyasaland laws.
alangidwe basi
apolisi timadalira inu amenewo chitani nawo basi.
paja alomwe ufiti nde wao.ndi ncthito yapakhomo pa munthu yomwe,mpaka atchulepo juju.
mafupa aawanthu saona za chilendo.zikasokonekera mukazipeza ku leba office kokasaka ntchito,anthu osasamba.
Apolice chitani nawoni ampala bwazi onsewa.tatopa ndikumva nkhani zaku manda.kkkkkkkkkkkkkkkk
Aphedwe aku Mozambiquewo.
thy killed a person they need t killed also. They removed someone’s flesh remove theirs too
yemwe amamugulisayo afunsidwe bwino. mwina inali deal ndie wangowapachika anzakeo poti anadulisa mafupawo. munthu sangango bwela kwa ine kut ndimugule mango pomwe ine sindidya mangowo. no smoke without fire.
anthu oipa awa alandile chilango chokhwima kuti wena atengelepo phunzilo chifukwa cha khalidwe loipali.kufuna kulemela mu njira yoipa ya chidule .kuchitabwino sathamangila ai anthu opepela lero dzawavuta.
iv
look at them. stupit.
It need to give them life in prison,anthuwa ndiwoipa osamawanyengelera.zilango zikumakhala zophweka ndichifukwa chake sakuleka moyo oipawu.
Last time a group of human bones sellers from Mozambique were given a bell of k20,000.00. This indicates that its not a serious offence. Can we revisit our laws. Shitiiiiiiiiiiiiiii Nyasaland laws.