LETS PRAY THAT SPIRIT OF PLUNDER IN MALAWI BE CUST OUT.THIS IS TOO MUCH-LEADERS AT THE4FRONT,SHAME.
pierra
9 years ago
this will no doubt fan the flames for the creation of a federal state of Malawi. It cannot be tolerated that a country’s population is jointly and severally punished for the fiscal embezzlement by the few.
what is required right now is a complete audit of accounts to find out the culprit districts and regions.
gloria
9 years ago
when nations says dowa he means the responsble persons in dowa who misuse the fund, whether ndi ku assembly or else where, are responsible to pay the money
Ramsey Majiga
9 years ago
” Kuthako kwa jongwe kumbaoneka tsiku ya chonzi” lero zadziwika….. kwawo gule wamkulu
Rodrick Mbuya
9 years ago
Abweza bwanji anthu aku Dowa oti ndalama amaba ndima accountant, DC, DPD ndi ena? I wish you could arrest these people not punish pple from Dowa pazinthu zomwe sanachite. Ndikuziwona kuno ku BK mmene ndalama zaboma zikubedwera ndi anthu ogwira ntchito boma. Munthu osauka ngati ine sindingabwezenze ndalama zoti sindinadye ACB ibwere ma districtmu idzagwire mbava zomwe zikuba ngati ku Dowa ndi Balaka
Ken Msoni
9 years ago
izi its because ma council kuyika maudindo un qualified pple like M’mbelwa DOA wa standard 8, amadula ma tikiti ku Likoma koma koma a Makileni kumupatsa u DOA ku Mzimba
Issa Kabudula
9 years ago
The problem we have in Malawi is that of lack of love of each other where a person if given meant of items or cash the only thing she/he thinks is to manage his/her own issues, for World Bank to ask for refund zopangitsa manyazi why a refund? Charity can not be refunded – the amount itself too little for Malawi problems. For us Malawi please lets learn to respect our positions other wise you deserve to be wiped out and the young boys and girls who are hungry for work and development to take over your positions.
Bwampini
9 years ago
Payback the money Malawi! Finish n klaa
Charter
9 years ago
nazoni!
Jacob David
9 years ago
Kodi mwaiwala kuti mabedi a ku Mponela Dowa hospital anapita ku mpoto? Madollar amenewa sanalowela konko?
LETS PRAY THAT SPIRIT OF PLUNDER IN MALAWI BE CUST OUT.THIS IS TOO MUCH-LEADERS AT THE4FRONT,SHAME.
this will no doubt fan the flames for the creation of a federal state of Malawi. It cannot be tolerated that a country’s population is jointly and severally punished for the fiscal embezzlement by the few.
what is required right now is a complete audit of accounts to find out the culprit districts and regions.
when nations says dowa he means the responsble persons in dowa who misuse the fund, whether ndi ku assembly or else where, are responsible to pay the money
” Kuthako kwa jongwe kumbaoneka tsiku ya chonzi” lero zadziwika….. kwawo gule wamkulu
Abweza bwanji anthu aku Dowa oti ndalama amaba ndima accountant, DC, DPD ndi ena? I wish you could arrest these people not punish pple from Dowa pazinthu zomwe sanachite. Ndikuziwona kuno ku BK mmene ndalama zaboma zikubedwera ndi anthu ogwira ntchito boma. Munthu osauka ngati ine sindingabwezenze ndalama zoti sindinadye ACB ibwere ma districtmu idzagwire mbava zomwe zikuba ngati ku Dowa ndi Balaka
izi its because ma council kuyika maudindo un qualified pple like M’mbelwa DOA wa standard 8, amadula ma tikiti ku Likoma koma koma a Makileni kumupatsa u DOA ku Mzimba
The problem we have in Malawi is that of lack of love of each other where a person if given meant of items or cash the only thing she/he thinks is to manage his/her own issues, for World Bank to ask for refund zopangitsa manyazi why a refund? Charity can not be refunded – the amount itself too little for Malawi problems. For us Malawi please lets learn to respect our positions other wise you deserve to be wiped out and the young boys and girls who are hungry for work and development to take over your positions.
Payback the money Malawi! Finish n klaa
nazoni!
Kodi mwaiwala kuti mabedi a ku Mponela Dowa hospital anapita ku mpoto? Madollar amenewa sanalowela konko?