Email a copy of '100 Ethiopians arrested  in Karonga: Five Malawi citizens nabbed for aiding illegal entry' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

28 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
kholowa mkabudula
kholowa mkabudula
9 years ago

ayi malo ndi ambili, enafe tinachoka kumeneko kudzakhala ma iligo kuno ku ingalande. Ndiye malo anga mumupatse mzibambo mmodzi ineyo sindidzabwelanso! komanso amalawi ena ndi ma iligo ku joweniko remember!

kholowa mkabudula
kholowa mkabudula
9 years ago

ayi malo ndi ambili, enafe tinachoka kumeneko kudzakhala ma iligo kuno ku ingalande. Ndiye malo anga mumupatse mzibambo mmodzi ineyo sindidzabwelanso! komanso amalawi ena ndi iligo ku joweniko remember!

eish
eish
9 years ago

I agree, Malawi is too small to have them in our country too!! eeyah, abwelele kwawo!!

andy mulipo
andy mulipo
9 years ago

ai imeneyi siyogwira fans imeneyi apane isadzayambilenso kungolowa basi akuona ngati malawi ndiyofiyira eti apolisi muwapane alire chiethiopia anthu amenewa.

unwarried officer
unwarried officer
9 years ago

Malawi is too small please let these people go back homes

Theba
9 years ago

Osawasiya akafika kuno ku joni amanyada amatilipira ma 300rand pa wk agalu amenewa,amatitenga amalawi ngat zitsiru.mission yao inali njira kt azibwera kuno ku south africa

MMALAWI
MMALAWI
9 years ago

sadamvetse amenewa amaona ngati game yalero ili kuno kumalawi.amabwera kudza chemelera mpira

Thomzey
Thomzey
9 years ago

Kodi madili zonyozana zachani amalawi akufunako madola munthu nmozi $_$50 kunfikisa Ku zareka nde ukanyamula 10 sibasi waoloka inu muziti atumbuka madilu anzanu akulemela osawanena a cashgat wa bwa akuyanbisa zonyozamitundu anabadwila muuhure alive bambo ati amupase mwambo

Dineo
Dineo
9 years ago

Kodi a MALAWI mumafuna kusangalatsa ndani? mudzasowa kothawira tu ndi nkhondo mukuphika ku mudziko, ndi sonkhana sankhana…. kuzunza ma Africans anzanu choncho? chonsecho akudzutsani pa AIR Malawi ndi ma ETHIOPIANS omwewo!. kodi mumati mukutani mukamatero? mumadziona ngati muli ku EUROPE? pa LAMPEDUSA kapena??? mxii! asiyeni anthu adzidutsa. and it is high time, a MALAWI tidziwe kuti mzako akapsya ndevu mzimire mawa azazima zako. mudzasowa kolowera inu sure ! mwina mudzakwera ndege kumapita kutsidya kwa Nyanja>…////////////////////////! kaya! change change ONE AFRICA for Africanss! kodi ndinu chiluma panokha?? za u goodgirl simunasiyebe?

Bwitoto
Bwitoto
9 years ago

Pali.za utumbukanso apa? Anthu ena anabadwa ndi uchitsiru basi eti? Shame on yo u man!!!!!!!

Read previous post:
Up up goes beer, soft drink prices in Malawi

Carlsberg Malawi Limited has increased prices of its alcoholic and non-alcoholic beverages by 14 percent and 23 percent respectively with...

Close