Email a copy of '7 secondary schools to be constructed in Mchinji – Mutharika' to a friend
Loading ...
Email a copy of '7 secondary schools to be constructed in Mchinji – Mutharika' to a friend
A six-member crew of oceanographers and tourism explorers has sailed off Salima beaches of Lake Malawi for a 52-day expedition,...
With all the building that APM is promising there won’t be sufficient bricks to meet demand. He needs to start building kilns now. Come 21 May he will have plenty of time on his hands to get building because he will not have to run the country; he will be OUT OF OFFICE!!!!
kkkkkk nophiya kkkkkk. ubongo.. iyi nde ija amati misala
Bwetule kunena ndowe.
kodi iyi ya ma salary a aphuzitsi omwalila wanenaponji dule iweee. nkhaniyi inayamba kaleeee zedi , ku education bwanina angathe kuthandiza kufukulapo ndi JOJI MKONDIWA, ife timangoona poti tilibe mau. kunali kugawana ndalama left and right. koma ma bizimizi, etc.ma junyozi kumangti mhu koma kodi zimatelo. tinganenenji akapompa ife.
ndalama za VISION 2020 gudall gondwe anali pa fore front. anthu ankangogundana mitu uku apita uku abwera. ma truck anagulidwa ngati akugula ngolo anthu.zinabookatu ndalama.
komaliza ose akuba ndikusunga cisisi anapatsidwa mipando yonona.
SUDAN-AL BASHIR
PERU- GARCIA
WINA AZIONASO PA 23 MAY
JUST BUID ONE TO BEGINNING WITH, SEVEN IS TOO MANY FOR DPP GOVT.
Uyutu wapenga misala ndithu!
APA NDIYE TIMATI MUNTHU WANKULU WATHA NZERU WAZINGWA, KODI AMENE AMAMULEMBERA TRASH IMENEYI NDI NDANI KODI SIAMAUNIKIRANA ASANAKALANKHULE ZOPUSAZO, ZIMENE ZIKUSONYEZA KUTI KU CHIPANIKO KULI MBUTUMA ZOKHA ZOKHA
chindere chakufikapo. dpp GUYZ you better pack up and GO!!!! come may21, 2019. MALAWI ANAZINDIKILATU. mabodza tinatopa nawo ife. MWADYA MISONKHO YATHU MOKWANILA
at what level is Mombera University now? voting mutharika into power again is like hanging oneself in your own house!
Akulu mutuwo koma ukukoka? Munanena kuti mukufuna malawi azafanane ndi Europe in 5 years to come. Then you said mchinji izifanana ndi chipata. Zigwira mutu?