Email a copy of 'Asu delighted to sign for Wanderers: Cameroonian says Malawi giants to reclaim lost glory' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Asu delighted to sign for Wanderers: Cameroonian says Malawi giants to reclaim lost glory' to a friend
A father of 11 children in Luwinga Township in northern Malawi who was working a security guard is under police...
chaka chino ndi chanyelele
Akuluakulu, munangozolowera kunyozana basi. Osangotsekula pamene mungathe kupeza za matimu anuwo ndikumapereka ma comment anu pamenepo bwanji? Mulibe zolemba za matimu anu kuli mphale zokhazokhako? Ifetu paja tinazolowera chikho chikangosintha timayenera kuchiyambirira kuwina. TNM Super League awonjezera money, tiperekezeninso kutsegulira prize money yatsopanoyi. Kugula ma players nkukhala ndi money. MANOMA go konko!!!!!!!!!
Tikuonelani season ikuyamba posachedwa!!!!!!!!!!!!!
am expctn’ alot from lali luban n hope not to expreance what l expnce last season.
We have to thank our executive for there jobs kkkkkk
Kwaoko ndi phale noma phuma kufera zina lakuja hahhaha!!!!
First of all, his real name is not Lionel, now look at Wanderers Chairman, he looks like a mini bus callboy. I wouldn’t take the people in the picture seriously, just a bunch of mini bus callboys.
Welcome to the Blue team your services will be needed & we hope you will contribute something to the Blue army…
Tachita bwino kutengako m’modzi yekha wakunja ifeyo cholinga chathu ndikuti tilimbikitse anyamata athu amomuno mu Nyasaland kukhankha mpira.
is this guy good enough? Malawi we like anything foreign. These are the reasons we dance to bubblegum music from Nigeria.