Email a copy of 'Atupele sets the tempo for Malawi 2019 elections: Addresses supporters at UDF headquarters' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Atupele sets the tempo for Malawi 2019 elections: Addresses supporters at UDF headquarters' to a friend
The main opposition Malawi Congress Party (MCP) has changed tune in the K4 billion “funding by-pass” which was allocated to...
Too late, MCP for change
This is the guying who is completely confused. He doesnot know what he wants in DPP let alone in UDF. If you want the party to be strong why sell it to crocodiles (Dpp). Atupele you are so opportunistic, you take malawians like cartoons
Resign first in the cabinet mwana wa mbava u want to increase ur bargaining power mugwela limodzi ndi goodal gondwe and nankhumwa mbava inu ana a mfiti Mia sakusiyani muvina agalu
KKKKKK….Like father like son zowonadi…Yathano five years mwayambapo…Munalitu chete inu ngati simumawona
My good friend Atupele consider your chances in the presidential elections very slim
Kodi inu a MCP mmangolubwalubwa, mudzachititsa liti kapena atsogoleri anu adzachititsa liti msonkhano, kuti tadzaone anthu ochuluka chonchi? Kapena tinene kutinso atola nkhani a nyasatimes ndi onga a MBC kuti akukukhomelerani, safuna kuti tione masapota ochuluka pa misonkhano yanu?
Bambo Atupele mwapusisa anthu kokwana.Chipani chisamakhale ngati choopsyezera mundale kuti muzipeza timanakinaki.Pano cabinet reshuffle ili pafupi mukufuna anthu kuti muzitolere.Mwadusitsa ma bill achabe ndikuzapondereza electoral reform bill kuti muzidya nawo ma cashgate wo.Pangani zomwezo kuti mudyenso ka 4billion kaja ka Goodall Gondwe ndi Nankhumwa.And mwakanikatu kuuza anthu zomwe UDF pachisankho iyima yokha or Ndi banja lanu ndi dpp?.Facebook ndi Whatsapp tiuzeni zomwe muli?Tisamangotengerana muthumba ngati malonda amphaka.
Mwana osapola liwombo komanso pa mchombo uyu. Moti iyeyu sakuwona kuti dzanja lalemba khoma. Moti baby ameneyu sakuwona kuti Lucius Banda naye akayambapo zake ndiye kuti mphepo ya mwera yalowa muchipani. Plibe munthu amene malimba ndi mphepo ya mwera.