Email a copy of 'Atupele still standing, UDF ‘new begining’ for Malawi inclusive growth' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Atupele still standing, UDF ‘new begining’ for Malawi inclusive growth' to a friend
Malawi Congress Party (MCP) first deputy president Sidik Mia is crisscrossing all the constituencies of the populous lake shore district of...
thupilose malungooooooooooooooooo.
1994 tate wake ndiyemwe akanaombola acinyamata kuti pofika pano bwezi zinthu zili patsogolo. but he was busy ndi maukwati ake ndi zibwezi, ku CI kumusi uko when he was sourcing every weekend parties to that whore jounalist, bust kuyenda ndi usiku ku cinyonga plus sourcing wa pakhomo then went on state wedding , then ku SA ,UK hospitals at last a state funeral under the finances of tax payers money. now tate wako is on back bench kukupopa. he blew up the chance
Ku Blantyre Rural musavotere anthu amene alephera kutimangira chipatala mzaka 55 zapitazi monga UDF, DPP ndi MCP. Sitingamakhale opanda chipatatla kwa zaka zonsezi. Ma MP onse alephera kubweretsa chipatala kwathu kuno ku Blantyre Rural musawavotere.
Mwadyaidya zaka zonsezi lero mukuti new begining wina akuti malawi watsopano. Paja ife tinkafuna supporr yanu ku parliament kuti mwina tipulumutse ndalama za boma UDF and UTM munkathandizila kuti president akhalebe ndi mphamvu pa ACB. Tsono mukubwera tikuvoternii kuti mukakhale ndi ulamuliro pa ACB mukatibere mokwana, mwauponda
We will try the best
Haaaaaaaa mwana wachepa bolamkuluwako awona lero iwe nachisale chododa gwira mchira wanga SKC motoooooooooooooo odi ukoooooooooooo
Atupele, this is my second advice to you. I am a strong supporter of UDF and when voting, I vote for president, MP and Councilor all for UDF. I don’t bother who has been featured. As long as he stands for yellow, I always support that one. No matter what UDF cannot win neither UTM will win. The battle is between the two Giants DPP and MCP. DPP has more chances of winning though. The way Mutharika has loved you during his tenure of office has impressed me. I have seen him not to be vengeful. And you will gain… Read more »
Iwe chitsilu eti. We do this for Malawians and not politicians position
Which Malawians iwe galu? Just keep quiet Mbuzi!!!!
Mvera mwana ndiwe chitsiru kwambiri do you think he is so poor?
We are not discussing poverty here iwe nyero. Did he join DPP because he was poor? Dander head.
VOTE WISELY VOTE CHAKWERA
Atupele just join Chakwera, it will help to stabilise your political career. The truth is you cannot win this years election, you lost your voters due to your political instability. Had it been you were stable, the whole southern region would have been yours not UTM.
You need to be stable, under Chakweras mentorship, you will surely rule this country – you have kuthekera kotero only if you are stable.
nawenso iwe takhala chete usatisokose sinkhondo yako iyi
Akagwere uko !
Munthu walakwanji? Wake up .its not time for miseche. but relate the points to what you have