Email a copy of 'Auditor arrested for beating his three dogs to death' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

16 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
RICHI
RICHI
5 years ago

KOMA SIBWINO KUPHA ANZANU KKKKK

URIM AND THUMIM
URIM AND THUMIM
5 years ago

UKADETI NDI KWA ZIWETO
ZOMWE ??? AGALUWO MWAWALAKWILATU —

Mungaba
Mungaba
5 years ago

Hahahahaha

Mungaba
Mungaba
5 years ago

hahahaha

nonsense boma ili
nonsense boma ili
5 years ago

palowa corruptionitu apa…. mpaka okupha galu kumangidwa kkkkk koma yaaaaa, muyambenso kugwila mikango,akambuku ng’ona ndi zinyamazina zomwe zimadya zizake mwa a police……

#DzukaniAmalawi
#DzukaniAmalawi
5 years ago

If the Police were able to swiftly deal with animal cruelty cases, how come they are unable to arrest criminals who are looting, killing albinos, killing each other and beating up spouses to pap. This is a true example of Police being in politicians’ pockets. They just look the other way. I bet the Auditor (after passing on the brown envelope) will be acquitted for lack evidence despite the fact the dogs are clearly dead. The investigator will “fail” to prove that the crime was linked to the auditor……..case closed!

WINIKO MASANGWI KALIATI
WINIKO MASANGWI KALIATI
5 years ago

Zoonadi a Malawi ambiri sitimadziwa kuti kuzunza ziweto ndi mlandu. Kumathamangira kusankha tiagalu tonenepa bwino wakwa neba akabeleka koma nkumakanikanso kuwadyetsa. Mapeto ake amangoyendayenga m’makwalalamu m’ma bin kwa anthu then amakalumidwa ndi wachiwewe kumafalitsa kwa ena or nkuluma anthu. CHONDE OSAMASUNGA ZIWETO NGATI SIMUNGAKWANITSA KUDZISAMALA. Mumalephera kusunga abale anu koma kumafuna kuweta agalu 5

Phwisa
Phwisa
5 years ago

Gentlemen a police ntchito yawachepera. Kkkkkkkkkkkkk. Zoona.

ade
ade
5 years ago

Those who murdered Chasowa are stealing walking free. The one who has “murdered” his dog is arrested.

KILINDABWITE
KILINDABWITE
5 years ago

Dziko liri mmanja mwa agalu.

Read previous post:
Fredokiss leads, other Malawi urban artists follow to hold free shows

Urban music artists have started to emulate Hip Hop act Fredokiss in holding free shows in the country. Fredokiss initiated...

Close