Email a copy of 'Baby dumper ordered to do community service' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

50 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
John Muhammad
9 years ago

Mayiyo mmene amakwerana nd mwamuna wakeo samadziwa kt apanga mwana,amangomva kukoma bas! Zitsru zawanthu!!

kammudoni
kammudoni
9 years ago

Nkofunikanso kuti bamboyo alandile zikwapu 1111 komanso azile ndi kusuka mite go 111, pomaaliza amwe mazi ndowa ziwiri osapumila, apo ayi akakhale pa shamba Ku chichiri kwa zaka 4.

nsanje port
nsanje port
9 years ago

Koma chisoni ndithu…mwana 3.8kgs kumutaya,anzanu abereka WA 1.8kgs uyu akupumayu

mwiza
mwiza
9 years ago

Komanso Bambo wake asese 20 hours kuti asamapereke Ana kwa anthu osasamala. Inu zowona
mimba kumamangopereka kwa amisala. Mmene kumavutila kupanga mwana muja.

Laurence Chrles Jelenje
Laurence Chrles Jelenje
9 years ago

amayi inu …need DELIVERANCE ndithu

Jando
9 years ago

Concealing death is a misdemeanour carrying a sentence of 2 years not 5 years imprisonment.

Tiko
Tiko
9 years ago

Wanangwa and Viva Nyimba. The names tell it.

Lumbani
9 years ago

If she belongs 2yo family rit. I dnt agree wt u a judge v dis matter. U better jst pool ha cold water unlyk kunyengeza anthu kt mwapeleka chilango. 40hrs community service? Shame on u Mr Judge

patrick
9 years ago

Dzomvetsa chisoni kwambiri kodi akhothi mumanya manyi pogamula mulandu kamba chani? kodi simoyo umenewo amautayao, komwe kuli kupha, tsono kachilango kameneka inu eni mukuti mwalanga? gudge wopusa iwe kwambiri ndipo sukudziwa kuti uli pamenepo kamba chani. Ndakhumudwa kwambiri iwe usiye mtchito.

Blessings mdeza
Blessings mdeza
9 years ago

Kod ma judge enawa ndi dzina lokha eti?kachigamuloka kachepa mayiwa amafuna kupha amayenela kulandila chilango chowamvexa kuwawa.

Read previous post:
Mutharika tells UN Malawi polls were ‘credible’: Obama tips on democrcay

President Peter Mutharika has told global leaders meeting in New York, US  that he was elected Malawi’s fifth Head of...

Close