Email a copy of 'Back to three-horse race for Malawi FA presidential polls: Yabwanya, Mijiga cleared to face Nyamilandu' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Back to three-horse race for Malawi FA presidential polls: Yabwanya, Mijiga cleared to face Nyamilandu' to a friend
The peaceful conclusion of the recent tripartite elections in Tanzania, and the smooth transfer of power from former president Jakaya...
Akuti mpikisano wa abulu atatu!!! Okweeeee!!! Si vi wa kambwe ivi???
I smell sombdy leaving a fam campus, why is it yabwanya was disqualified, just shows there ismismanagement of fam reasources, once yabwanya will take a seat, the following week it will be auditors showing their talents to catch a aman so called walter.
Tiwoneko zina.
Three-horse race ? enawo ndiye ayi akanakhala kuti panali anthu ena odziwa
(Chibowa,Botomani, Somba ,Jack, Kinna etc) koma pa list iyi bola Walter yemweyo
Kodi inu amene mukufuna Wota, ndichani chomwe iye waiwala kuchita muzaka 12 zonse wakhala pa famu pulezident chomwe akufuna achite zaka zinayi zikubwerazi? Zopusa basi ngati mumadya naye ndalama zakuba kagwereni uko, anthu wodzikonda inu. Iam against the Appleals Committee in Mfune, here in Malawi we start to produce academic qualification even during interviews, ndiye zongofuna munthu awonetse professional qualification zayamba liti? Those inconsistencies are killing our education standards, alibe MSCE alibe basi sizobisalira kuti ali ndi Diploma ya Community Development basi ali azipita ku famu hoping Malawi football to improve, mwanyika. By the way did Madise the lawyer go… Read more »
Its now a 3-horse race!!!! Can i prophecy!!Prophecy Major,Major! Who has an Ipad here?
I want to take a photo for FAM presidency results! I see a giant who speaks like a hornet (bembelezi) falling here!!! whoooooooooooooooooooooooooooooooooooooooooooooo!
Ant nyamilandu
zaziiiiiiiiiiiii
Mumafufun alowe unopposed. Nyimbo yimodzi samachezera gule tione zina abale panopa ambiri alibe chidwi ndi mipira yathu koma ya kunja kamba momwe zilili pano let us change give others chance no life president of famu
Wonyamilandu no chance must go and squander illovo money not money meant for development of soccer in malawi,you have killed malawi futubo nosense!