Email a copy of 'Balaka again! Malawi Police arrest teacher for sexual assault on pupil' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

40 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
ehnest ngonyani banda
8 years ago

koma guys penapake lets use our common sense zoona munthu 44 yrs kukakomedwa ndi kamwana ka 11 yrs,thats bullshit vuto lake mijombo mukapalitsa palitsa mipaliro yanuyo mumaona ngati mwafikapo basi.but guys lets respect our sociaty

The blood of duwe
8 years ago

everything ku balaka wats wrong with u there behave urself pls

aurora
aurora
8 years ago

zimamukomela thats y amangopitapitabe kwa teacher ko….fodya et

John
John
8 years ago

Mwana wa standard 3 zoona, ma guy ma hule onsewa? In Malawi, you can screw as much any size, colour, shape etc.

Prodigalson
8 years ago

Mwanayo anatopanazo?Bwanji sanaone tsiku loyamba kuti ndi zoophya koma wadikidira mpaka kumukulisa nanyongo ndikumaulula bwino?Kungoti apa chilipo chomwe anthuwa anayambana basi.

professor_steven_Nk
professor_steven_Nk
8 years ago

what on earth”””|||::@@@@@@@ koMA ANTHU ENAWA AMAGANIZA BWANJI MPAKANA PAMENEPO…. NO NEED OF GOING TO COURT FOR DISCUSSIONS JUST ARREST HIM….. NO PROCEDURES…..

WAMANGIKE AMENEYO

Khwethemule
Khwethemule
8 years ago

Midyomba sizodabwitsa ndi khalidwe lanu anthu akumwera. Zigolololo too much. Mtsikanayunso zimamukomera osaulura first day bwanji? Because of jando u teach your children to have sex with elderly people from a tender age. This 11 year old knew what she was doing. Anavinidwa kale ma offals am’bamboyo samamudabwitsa mwanayu akuzidziwa kale otherwise akanaulula first day. Southerners are a disgrace to Malawi. 11 years in standard 3 zoona? These days?

Binton wakale
8 years ago

Izizi anyamata amasiku ano ziziwachitikira kuumira maningi ndawa.Nanga inu munthu paka zaka 44 osakwatira amatani? Ifeyo pamenepo ndiye kuti tili ndi ana atatu kapena awiri.Anyamata inu akazi sapha munthu zikwatirani panthawi yake mofulumirako kupewa zoterezi komanso ana amakula bwino bambo ukadali mnyamata wamphamvu.Uyuyu just look suppose he marries today mmene mwana aziti 10yrs old basi bambo akuchita retirement approx 55 to 57yrs.Anyamata moyo wanuwu simukuganizira bwino komanso wabanja lanu.Ana amafunika akumvetsetse kholo kukoma kwazaka zingapo.Komanso mkazi amvapo chani ukwati 10yrs munthu ukalamba wayambika?Wake up anyamata mukutichititsa manyazi kwajinji.

Murray
Murray
8 years ago

Balaka Balaka………why? she is your daughter sir.
Komanso m’Balaka alimotu mahule otchipa, bwanji osatengako mmodzi?
Plz timatumiza ana ku Sukulu kukaphunzira osati kukakwatiwa

rachel
rachel
8 years ago

Athu Otelewo Azilandilitu Sentence Osachedwa Nao Mucastody Ayi Life In Prison Basi, Ameneyo Silast Born Wake.Male Teachers Muzikhala Ndi Umuthu

Read previous post:
Head count exercise scare Malawi civil servants: Crackdown on Ghost workers

Malawi government decision to head count each and every civil servant has met with resistance from some quarters amid fears...

Close