Email a copy of 'Bamusi warns PAC indaba against resignation calls, ultimatums for Malawi President' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Bamusi warns PAC indaba against resignation calls, ultimatums for Malawi President' to a friend
Malawi Police in Chiradzulu are keeping in custody a man for allegedly killing his 12 year step daughter because she...
Haha this Bamusi guy is a clown. He is talking about pointing fingers . Really Bamusi? This man is forgetting that his administration has been blaming everyone else for the economic problems our country is facing. Isn’t it funny now he does not believe in finger pointing? What a hypocrite.
ladies and gentlemen aside Saulosi amuna amu DDP ali beautiful chaponda, bamusi, mwanamveka, mussa, the list is endless ujeni uyu kkkkkkk
MABVUTO NDI MABVUTO NDITHU.
Mavuto Bamusi ali buuuuu kutuwa ndi modza ngati mafuta kulibeko ku DPP
Guys, Musiyeni uyu Bamusi, mwana wosamva
A Bamusi ndinu achitsirunso dele.
Mabvuto Bamusi is one of the useless guys who are betraying our clueless president. You better sgut up your stupid mouth Bamusi otherwise you are making us more angry with your senseless talk.
There was a time when the likes of Mabvuto Bamusi, Collins Magalasi used to feature on MEJN program trying to articulate economic issues. I took them for intelligent people. I was wrong. Now they are both president advisors and I wonder where all that has gone especially against the economic turmoil the country is going through. Too theoretical!
Bamusi ndi munthunso yemwe samakonda ziko lathu la Malawi, Kamuthu kadyera kwambili. Cholinga cha Bamusi ndikukhala pa udindo basi or Amalawi onse atafa kakhoza kukakamira udindo. President Peter Muthalika ndi wabwino kwambili, koma anazungulilidwa ndi anthu oyipa kwambili okonda udindo kuposa dziko lawo. who dont care about Malawians, unpatriotic thugs; but udindo basi. Afiti, ana anjoka, Alusifara, ana a beliyali, Dzinkhanila dzokhadzokha. Kuchita kupangira kondaine kuti adzisankhe unduna ndi u adviser. Kumangompasa Chidima Nsogoleri wathu kuti asakuchoseni udindo. Olo lero Bill Gates atati apereke $5 billion yothandizila malawi koma achepese ma advisers zikhoza kukana. cholinga zilamulire basi. AGULUKUNYIDA INU
Iwe bamusi! Mutu ngati chibhama. Who are you to gag freedom of expression. Wakhuta mbwanda eti. Zingophwisa uko!