Email a copy of 'Bishop Mtumbuka opens boarding secondary school in Nthalire constructed by Catholic church' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Bishop Mtumbuka opens boarding secondary school in Nthalire constructed by Catholic church' to a friend
Government, through the Attorney General Charles Mhango, has said the implementation of the 2017/18 Farm Input Subsidy Programme is on...
Well done Bishop and congratulations.
M’bale Khima osadandaula ndi mchitidwe wa mapente, muwafunse a Chakwera anali komweko. Atakhala mtsogoleri wa dziko muyembekezera zomwe mwadandaulazo kukhala government policy.
Kwalero tiyeni tingothokoza a Bishop athu chifukwa cha masomphenya awo abwino.
Good news indeed. Kumanga sukulu m’malo akutali chonchi koti kuli maphunziro ochepa ndichinthu chanzeru. Mulungu apitilize kukudalitse ekleziya katolika kuti ufikire anthu ochuluka. I love the way catholic church invest in education. Atati amipingo ena ili mbweeeyi akupanga chimodzimodzi m’madela osiyanasiyana bwenzi zilibwino. Tisamangolekelera boma lokha likungodya ndalamali. Mukaphunzitsa anthu ochuluka mpingo wanunso udzakula ndipo opereka chuma kutchalitchiko adzachulukanso. Sizomangogula ndege , ma galimoto ndima suit. Give back to the poor who try so hard to give the little they have to church
Positive news from the so called cursed nation…kudos the Catholics..inu ama Pente mukutani apart from ripping Tithe from poor masses??? kumangogula dzimagalimoto