Email a copy of 'Blantyre Water Board choked by K10bn debt: Suspends cash outflows' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Blantyre Water Board choked by K10bn debt: Suspends cash outflows' to a friend
Malawi Police in Lilongwe have arrested and are in keeping in custody three Indian nationals and one Malawian accused of...
Do we audit these institutions? Do we use the results after auditing? Malawi will never develop until we have a system that is genuine and working. A system that checks and acts when wrong things are done. ODPP nayo ntchito yawo ndikupeleka ma certificate not checking and verifying contracts.
wasting money on allowances and seminars especially senior management
Poor management, Blantyre water Board
Pasavute. Let them hold ‘a Water night” at Sanjika Palace and invite DPP to attend. Upon attendance, DPP will have to be asked to sit next to the President and contribute to the course. Ntchito za chifundo izi a DPP, nanga zifike potimwetsa bibi a mchimbudzi boma losamalira anthu liripo?
Mwaonatu, muli ndi ngongole thooo koma kumapereka ndalama ku DPP, ana anjoka inu osakonda dziko lanu. Mumamvera matchona cholinga choteteza ntchito zanu. Shame.
A Bakuwa 128 million munaba ndi anzanu aja inakatha kukuthandizani kubwezako ngongole zina.mbava iwe!
Too much kuba anyamata aku BWB. I have no sympathy to BwB people. Kunamizira kuvuta mmakomo mwa ma customers kudula madzi ndi ma fake bills anu kumbaliku mukuba… am not surprized.
Mavuto is Blantyre water board management is very disorganised, we have never heard blantyre water board in the papers for financial problems, there is something wrong the way it is run currently, Boma needs to take action or the current management will take this board to bankruptcy
Chief Executive officers in Malawi. Koma ntchito yanu mumayiziwa osati nanuso mutimwese madzi abibi. Blantyre cant allow such madness
Chief Executive officers in Malawi. Koma ntchito yanu mumayiziwa osati nanuso mutimwese madzi abibi. Blantyre can allow such madness