Email a copy of 'BLM promotes safe sex in new Manyuchi condoms: ‘Tseketseke for Life’' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'BLM promotes safe sex in new Manyuchi condoms: ‘Tseketseke for Life’' to a friend
The Malawi beach soccer team on Saturday endured a bad day in Seychelles in the first quarter of the inaugural...
hahahahaha nanunso a Sarah zoona kupanga komenti zimenezi? tangofunsani ngati akazinso alipo makondomu, kuti uzigwiritsa ntchito.
koma ka mzungu angakayike mukondomu,wausilu mzungu ameneyu eti.anthu atopwetekana kondomu ili m’manja.kodi mwatosowa zonena eti?
Uchimo kuwuika pabwalo sopano!!!!!! Ankhu amenewa ayenera kuti akayesa kugwiritsa ntchito ndi azimuna awo makondomuwa, chifukwa ndi zodabwisa kunena kuti ndichokomesa chisembwere anakachiyese.
Comment Is This True?
These are the agents of death cunningly promoting adultery,promiscuity and the HIV in the guise of safe sex, reproductive health and safe motherhood.
Eeeeeeeee guyz chakachino kuli kunyenga akazi ambiri…. Wina alira.
ife sitivala condom ndife achimidzi
KOMA MANYUCHI MAKONDOMU ABWINO NGATI AWA SINDINAWAONEPO INE…. NDINAYAMBA KUGWIRISA NTCHITO KWA CHIBWENZI CHANGA CHOYAMBA NDILI PA BANJA KALE MPAKA PANO SINDINASIYEBE MANYUCHI….BIG UP BLM
Haraam
Amai Mitochi mubwere ku Big Brother tidzacheze, tiyese zimenezi basi tione m’mene zimako mera, nanga nkutani