Email a copy of 'Bushiri ready to employ Malawi Police officers victimised for Mzuzu crusade' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Bushiri ready to employ Malawi Police officers victimised for Mzuzu crusade' to a friend
Malawi President's Peter Mutharika appetite in spending tax payer's money in time of social economic and political doldrums, continue to...
Police were there to protect the citizens of this country as well as anyone who attended the crusade, Malawians should learn to stop politicizing anything.
Major just pray for holy ghost fire to come down and consume all those involved in transfering innocent police officers. By the way why din’t u see a vision and came up with a prophecy ha ha ha ha ha haha ha ha ha ha ha
Joy Moisture, you are saying truth Malawians we are too much jealosy thats why we are poor, Amwenye being foreigners are rich because they do promote each other.
iiii, boma la pitala safuna ena atukuke
uneneri ofuna ulemelero wa dziko ameneo ai mateyu 24v 5-13
A Malawi chimavuta ndi nsanje, mzathu akamachita bwino sitimakondwa. Refer to our national anthem.
Bushiri sanayambe ndale….inu a Wright German kumamvesetsa zinthu!!
Bushiru is a man of God please my fellow Malawians lekani kunena azitumiki, ngati aprophet Bushiru ali oyipa abwinonu mulikuti? Inu atsogoleri athu muboma chonde tiyeni tiwalandile a prophet S.Bushiri anthu amenewa akakala mudziko amatandiza dziko foreign exchange ndizitukuko zosiyanasiyana. ngati kuli Kuweluza musiyileni Yehova, chimodzi ndichiziwa ine prophet Bushiru is a man of God ngati akulemela mumphamvu yasatana potchula dzina la Yesu mnazalayo ndekuti ufumu wasatanawo wagawikana. David anawopa kuchitila Sauli choyipa kamba koti sauliyo anali ozodzedwa wa Yehova, lekani kuchitila anthu a Yehova zoyipa.
Dear Prophet Shepherd Bushiri help me in everthing which I tried I failed why?
All the best Bushiri when did you leave pretoria go to malawi.so why do you need some security.Its only Almighty God who can protect you