Email a copy of 'Bushiri sending back Malawians working for him in South Africa' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Bushiri sending back Malawians working for him in South Africa' to a friend
Abida Mia, wife to first vice president of the Malawi Congress Party (MCP) Mohammed Sidik Mia, has donated K500 000 cash to...
BUSHIRI DID NOT COME TO MALAWI TO CONDOLE THE BEREAVED FAMILIES WHY? Nyasatimes answer on his behalf now
SOLDIER ON THE BATTLE IS NOT YET OVER !!
Cash crisis iyi. Osanamizira zimenezo ayi. Just indicate kuti cash flow siiri bwino so you are cutting on costs. This is normal to any business. It attracts revenue at first then the business starts to decline. And this being a church built on lies it cannot survive the test of time.
Don’t stop doing good, if the people don’t recognized your help and love.God has seen your heart
WHATEVER A MAN OF GOD DOES WILL BE APPRECIATED BY GOD. .MPHOTO ILI KUMWAMBA OSATI PANSI PANO.
Masiku omaliza,,tikhale ochenjela ngati njoka
We are told this is not the official position but advice being given to Mr Bushiri. I doubt that this advice has been adopted as it does not sit well with his other actions.
munthu wa mulungu satopa. akudandaula kunenedwa anzake yesu anakwapulidwa mpaka pa mtanda.. anthu ochimwa apempherereni..
How do you mean “you have done a lot for Malawi” ?
Bushiri is not seeking praises He is only saying zomwe a Malawi amamunena pomwe he only delivers good to them Mtundu wathu ndiwokanika. Akayamba kunena zamabodza, kuyipitsa za munthu amachita kupatsirana ngati chipako.. Wopanda woleletsa. Mchifukwa sititukuka tadzala mtima yoyipa Mukamawerenga bible mumapanga criticise phareeses . Simukusiyana olo pang ono If it was today yesu akanachulukitsa mkate ndi nsomba pamalawi pano mukanadya? Satanic eti? Mkamwa mwa nsomba kutengmo ndalama, satanic? Ambuye Yesu anati mudzapanga zoposa izi Woyenera kumuyikira red carpet pakati pa president wadziko ndi yemwe watenga anointing of God ndindani? Am not Bushiris church member Koma a Malawi mmmmmm… Read more »
You can say this again and again, Mtundu ovuta uwu waMalawi. Too much jelousy, kaduka, NSANJE ndi imeme ikuvuta pa Malawi.
Thats why even in our national anthem, jelousy is considered to be one of our enemies. Malawians are full of jelous pipo. u cant do anything good and be priased. Even during jesus’s time, jesus drove out demons and those who claimed to know God(the pharesees) said HE got his power from satan…Beelzebul. Malawians sitifunirana zabwino
Ife a ku banja la a Gondwe sititha kuyankha pa nthawi ino tidakali pa chosoni, m’bale wathu Ben lero akukanidwa poyera kuti samagwira ntchito Kwa Bushiri. Tizakuyankhani tilachoka mu nyengo iyi ya maliro.