Email a copy of 'Buyer shot dead over K200, 000: Malawi Police intensify investigations' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

37 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
max chapitah nchalo.
max chapitah nchalo.
8 years ago

Akuba inu mverani kuba muleke mukapitiza muona polekera.

nkrumah
nkrumah
8 years ago

Pliz police shoot to kill is the best policy for Malawi . If NGOs and court are disturbing you , do not we shall deal

Jimmy juga
Jimmy juga
8 years ago

Zikunyansani bwanji ena a police akugwidwa kuphananso nokha

Pasipawo
Pasipawo
8 years ago

Nkhanza ndi umbanda siyani tsiku la 40 lizakukwanilani

sinja wamasinja
sinja wamasinja
8 years ago

GIVE US OUR OWN SECURITY IN OUR NEIGHBORHOOD MR PRESIDENT

kamfana
8 years ago

ZIGANDANGA INU, KODI MUNAKHALA BWANJI?KUM’BERA MUNTHU KOMANSO KUMUPHA.SATANA WAMKULU.SINTHANI,FUNANI NJIRA ZINA ZA BWINO ZOFUNIRA NDALAMA.

apundi says
apundi says
8 years ago

anthu muziyankhula bwino zilizonse mumangoti apolisi akuba nawo, ife tidzakusiirani ntchito muzakhale ndi bata mmalawi muno, ife apolisi zimatinyasa kwambiri

Chiyendausiku
8 years ago

Abale mpaka munthu kumupha chifukwa cha k200,000 basi komanso munthuyo siyake so sad RIP

Esther banda
Esther banda
8 years ago

Ubututu basi

Kholophete
Kholophete
8 years ago

Mfufuzeni Supervisor. He deliberately gave the guy the money in the presence of people to show off komanso atha kukhalanso yemweyo we have people who could give you money and later send thugs to rob you of the same money. Cholinga chopelekera pagulu amafuna kuti ndalamayo ma thugs akakayitenganso, mnzake adzalephere kunena kuti waberedwa amafuna gululo lizizaikira umboni kuti analandiradi ndalama mnzakeyo. Stupid supervisor waphetsa mnzako.

Read previous post:
Malawi sex workers to get compensation over forced HIV tests

Malawi High Court has ruled that 11 prostitutes who were forced to take HIV tests by police six years ago...

Close