Carlsberg Cup semi-finals to be played at Kamuzu Stadium and Civo Stadium
Football Association of Malawi has released the venues of 2015 Carlsberg Cup semi-finals involving Big Bullets, Silver Strikers, Mighty Be Forward Wanderers and Moyale Barracks.
According FAM Competions Manager, Gomegzani Zakazaka, the first game will involve Big Bullets and Silver Strikers on Saturday ( 15 August 2015) at Kamuzu Stadium.
The second semi-final will be Mighty Be Forward against Moyale Barracks at a neutral Civo Stadium venue in Lilongwe on 16 August 2015.
Zakazaka said all is set for the semis and urged soccer lovers to patronise the games.
Meanwhile, the Nomads are not sitting idle ahead of their game, as they will play Fisds Wizard in a friendly match this Saturday at Kamuzu Stadium.
Sizoona
Bullets in ma mind
A FAM zitsiru za a2 Walter should step down ndamene apangisa zosezi.
Kkkkkkk inu a shocker simumadziwa za mpira,its semifinals the look on security and patronage of pipo.the spouse nawonso amafuna money mukufuna akamenyele Ku tchile ngati kumeneko anga kalipile 1000 ndindani,osadzanenaso mau amenewa anthu adzakusekani
Noma forever
Noma yanga woyeee!mabanker tili nanu
Woza!!be4 wanderers my favourite team.Fixture ili bwino kwa ife!!ma banker tili pambuyo panu!!!!
Gwaladi ndi wa Noma kuyambila kale..
Pa Carpet Nde Ma Banker Amaukatu, Bb Mukathamangitsdwa Molapitsa Pa Kamuzu Stadium Tikupezani Konko Kaya Akubelekani Kaya Ayi Ife Tikubwera Konko Koma Why Nama Vs Kaning’ina Lions Playing At A Neutral Venue? Asiyeni Akamenyele Ku Mzuzu Or Ku Bt Otherwise The Match Is Being Fixed, Apapa Mukukokela Noma Ndi BB, Mukiyendetsa Silva Komaso Moyale Ndi Cholinga Pamene Noma Mwangoibweletsa Ku LL Chiphamaso Mukuziwa Chomwe Mukupanga Osatipusitsapo Apa Komabe Tikamenya Bola Mwaziwa Kuti Mwatchela
FAM and Carlsberg mwakhwana heavy. Ife tufuna Bullets v Wanderers in final. Its very obvious if Wanderers would hav lost to Moyale if the game was to be played in Mzuzu and similarly Silver would have whipped Bullets if the game were played in Lilongwe.