Email a copy of 'Catholic Bishops start solidarity visits to flood victims in Malawi' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

36 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
mwai
mwai
9 years ago

Keep it up and may the almighty Holly Father keep on blessing his church

Mfalisi
Mfalisi
9 years ago

Koma akatolika otchuka mu ntchito zawo alipo pa malawi. Raphael kasambala, paul mphwiyo, thereza namathanga senzani, mwa ena. Sithole naye ayenela kukhal mukatolika malingana ndikuti Mchinji ndi ku chimake cha katolika.

Nyamithuthu Flood Victim
Nyamithuthu Flood Victim
9 years ago

A tear of Joy stands in my eye. . . . . .

Zefania Kabotolo
Zefania Kabotolo
9 years ago

Zikomo kwambiri kwa akristu nonse Akatolika popereka nsembeyi. May the Almighty God
bless you.

Nkhalamba yopanda mano
Nkhalamba yopanda mano
9 years ago

Mpingo woyera,wapamalo ponse, wofumira kwa apostoli. Nthawi ino yokumbukira kuzunzika ndi imfa ya Ambuye Yesu pamtanda, chitani ntchito zachifundo – kupemphelera, kuyendera, kudyetsa ndi kuveka anzathu ovutika ndi madzi osefukira mdziko muno. Ambuye azikudalitsani nthawi zonse atumiki a Mulungu!

Mbwiye
Mbwiye
9 years ago

Mpingo wa pamalo ponse wofumira kwa apositoli, womwe ukusunga manda a POPE woyamba Simon Petulo ku Vatican. Unamanga ma sukulu ponse ponse, unamanga zipatala ponse ponse, umalangiza boma kuti liziyenda bwino osamangosokosa zopanda nzeru ai. Komanso boma likamapanga zachibwana umalemba ma pastoral letter osati amasewera ai. Lero mpingowu wayamba ulendo wodyesa nkhosa za ambuye zomwe zavutika ndi madzi. Bravo catholic, bravo akrisitu ndi ena akufuna kwabwino omwe anasonkha nawo billion kwacha imeneyi. bravo boma polola ufulu wa chipembezo.

Happy Eduardo
Happy Eduardo
9 years ago

Yes, holistic approach of Jesus Ministry. You are setting a good example.

MELINDA
MELINDA
9 years ago

GOOD JOB AUNCLE

Mu umodzi muli mphavu
Mu umodzi muli mphavu
9 years ago

Eeeeeeee, khristu

muonosile
muonosile
9 years ago

Osangopita kothandizako bwanji mpaka kulengeza. Pochita ntchito za chifundo chimene dzanja lako la manja lichita chisadziwike ndi lamanzere.

Read previous post:
Wanderers donate to Bullets: ‘A friend indeed’

Mighty Be Forward Wanderers on Monday buried the bitter rivalry with Big Bullets when they donated K200,000  (US$444) to Malawi...

Close