Email a copy of 'Catholic give humanitarian aid to flood victimsin Zomba, Machinga' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Catholic give humanitarian aid to flood victimsin Zomba, Machinga' to a friend
Malawi netball giants Complex Tigresses will Saturday clash stubborn Diamonds in a grudge encounter in the finals of the OG...
kodi thandizo la anthu a Mulungu amalengezetsa? Amati pamene nkono wakumanja ukupereka, wamanzere usaone. Do not be like politicians. Kuzolowera kupembedza mafano eti?
@mlongoti….. Eish ! Koma na Amboni woka ananyanya . I have never heard kuti apanga donate katundu wofunikira apart from kuyenda komo ndi komo distributing ma comics or pamphlets. Zaziii.
Chonde Pano musayerekedze kubwera panyumba panga with those ‘ James Hardley Chase ‘ pamphlets chifukwa Ife tikulira pankhani ya ma floods
As a catholic,am impressed.Bravo catholic church.
Nanga inu mapastor ndi bishop oyendera magalimoto opuma monga Benz, Audio, GMC, Ferari, Fortuna etc muthandiza liti? Ndi mipingo yanji yomangopezeka mtauni?
Kwao nkulemba zakutha kwa dziko ndili alemba kale,isati kuthandiza nde wamboni ameneyo
Now,let us see if Rome will remember you to take over Zomba diocese. Fr. Peter, who knows, perhaps this will bring you some lucky. For Mzuzu, hoping Fr. Kim will take it!!!!
a mboni muthandiza liti?
Ife amboni sitithandiza koma kuthandizidwa ! So please don’t bother us