Email a copy of 'Catholic University of Malawi students suspected of murder after pub row' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

22 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
Binton wakale
8 years ago

Level yamaphunziro anu anthuni ku University ndiya utsogoleri mukakayamba zintchito tsano muyenera kumazolowera kukhala ndi anthu and tazionetsani kuti ink yambiri yili ndi zipatso zabwino ndithu.Pena ndikumadabwanso zikuchika mudziko la Malawi palikusiyana kwakulu zedi ndi maiko ambiri becoz masiku ano you know we have televisions tikuphunzira ndi kusirira ubwino wa anthu ophunzira bwino.The more anthu akamaphunzira dziko lima kwera miyoyo ya anthu koma with Malawi its opposite,kalero kuli anthu ochepa ophunzira this country was wonderful pomwe lero ink zambiri koma useless ndipo muzimvere chisoni nonse you are doing nothing than kuononga dziko sitikudabwa nanu ayi.Kuphunzira kwaku Malawi ndikomweko if you… Read more »

J b
J b
8 years ago

Akapitiliza tibweza chipogwe cause kaya munthuyo analakwisa koma tikuyng’ana kuti wataya moyo cause of kumenyedwa ndi maduka ndikukamutaya pafupi ndi nyumba za FIC

chirunga intellegesia
8 years ago

Mutipeze kuno Ku Chanco…ana osasamba inu . Kulimbana ndi ma pelli basi

konyopi
konyopi
8 years ago

mmm zovuta..munthu uyu amakamila ndeu uyu..I was there…RIP

Mdzukulu
Mdzukulu
8 years ago

I do not know if the law will be applied to them,being some of them,nephews and nices of bishops,priests and sisters. Let us wait and see!!!!!!!!!!!!

Mirella K
Mirella K
8 years ago

Ana akusukulu ya Ukachenjede ya Katolika (UkaKato) hei! Izi olo ife amene tili ku University yeni yeni (UNIMA) bambo,sitipangepo! Ife timangophuzula ndikugawa mimba mwaChikandamu koma sitipha! Silly stupid ana opanda nzeru nchifukwa chake simuli ku University yeni yeni !!!

M E C
M E C
8 years ago

NAGULU A CHINA MPHWIYO NDI KASAMBALA AMENEWO

ZIGAWENGA ZA MA DEGREE AWO

NDI MAPOLOFESA
MUNTHU WAMBA SIMUYESA MUNTHU !!

Mlauzi
Mlauzi
8 years ago

The problem is not the location of the college. In fact being in the rural setting would mean a conducive environment for study, away from the hustle and bustle of urban activity. I have been to this college and noticed how students guzzle, and are generally unruly. As others have commented, this is a capital offence. Let the law take its course

nkhedu
8 years ago

wasted generation

Mbobi
Mbobi
8 years ago

catholic university must just build a common room so that students must drink there and relax koma kumamwa mowa ndi anthu ammuzi mapeko ake amakhala amenewa a student ndimunthu wovuta kumumvesa!

Read previous post:
Macra issue mobile operator licence: Lacell to roll out ‘quality services’ in Malawi

Malawi Communications Regulatory Authority (Macra) has formally issued out a 10 year licence to mobile telecommunication service provider Lacell Private...

Close