Email a copy of 'Chakwera as an MP has right to ask questions - Speaker' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

7 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
Mesimadzi
Mesimadzi
5 years ago

The man has now realized kuti uphungu (u MP) ndiye saizi yake osati upulezidenti. Upulezidenti ndi wa ma big ngati achina APM. Kunsaila wamupatsa mkuluyi pressure mpaka kukumbuka ntchito za MP. A Chakwera kubwera ndiye kumeneko osati zochita mademo posapota zoti amuna azikwatirana amuna okhaokha kumuthandizira Trapence.

Ndendeuli
Ndendeuli
5 years ago

Uyu athera pa u emupi pomwepa. Can never rule Malawi

Omex70
Omex70
5 years ago
Reply to  Ndendeuli

Ndendeuli, ukanakhala kuti umawinitsa anthu ndi iweyo komanso kuti Mulungu ndi mbale wako ndikanavomereza zomwe wanenazo. Koma poti suli zonsezi ingokhalani chete.

Mulopwana
Mulopwana
5 years ago

Failed Reverend cum politician wanting development in his area? Ndimayesa mumungokhalira kutsutsa paja. Lero mwavomereza kuti 4 billion igawidwe ku ma constituency anu mwaona nthawi yatha. Mwaiwala mwezi wazana munali pa nseu ndi ma CSO kukana same money. Hypocricy

Phiri
Phiri
5 years ago
Reply to  Mulopwana

What are you saying you DPP supporter? za zii zopanda park zopanda Mchere! What is wrong with asking for development project?

Omex70
Omex70
5 years ago
Reply to  Mulopwana

Umbuli siwabwino. Mukuonetsatu umbuli bwana mulopwana apa. Anakuuzani ndani kuti munthu wa Mulungu sayenera kutumikira dziko kapena anthu?

Maunits
Maunits
5 years ago

His Excellency the state president 2019 May 22 has asked the question.

Read previous post:
MPs want K4bn Constituency Development Funds by December

Malawi's 193 strong member National Assembly on Thursday unanimously passed a motion to allow government disburse for utilization all budgetary...

Close