Email a copy of 'Chakwera blasts Mutharika, salary hike ‘unethical’: Malawi in crisis' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Chakwera blasts Mutharika, salary hike ‘unethical’: Malawi in crisis' to a friend
Malawian Vice President Saulosi Chilima has called on Malawians to develop hard working spirit and refrain from depending on handouts...
He too should not accept the increament to demonstrate that he means what he says. Other wise all hear turn to mere noise.
Losers MCP
A Mutharika sangayendetse dziko. Timadziwa kuti m’bale wawo uja adaliko ndi nzeru osati awa ai. He is so slow to think, imagine the way he talks and articulates issues, he is so empty and numb. Mulungu amafuna a Malawi tiwone kusiyana kwa mtsogoleri ndi mtumiki. Mtsogoleri amachita zokomera iye, pamene mtumiki amachita zokomera anthu ambiri. Awa sangatithandize. Koma zili bwino zedi chifukwa tibvutika tonse pamodzi ndi amene amapanga phokoso lokondwera kuti Pitala wawina. Boti likumira iri. Otithandiza aja tiyiwale sangabwere ai chifukwa tisayiwale kuti Boma la DPP ndilomwelo lidathamangitsa azungu aja. Lero mukuwafuna, zibwana eti? Azingopha nthawi mpaka tifinyika eeeeeeeeeeeeeeee!!!!!!!!!!!!!!!!!!… Read more »
chakwera is right
Munakana anthu abwino kufuna mbavayi (APM) ndiye mukulira chiani a Malawi, tiyeni Nazi simunati mudziwaso
very disappointed and disgusting,i mean realy,poor Malawi.
You malawians! U don’t know what you want, u already rejected Chakwera, you’re fools.
Stop complaining that’s wat you voted for
Chakwera is a hypocrite, he is receiving his new hefty salary.
Amalawi majority ndi kupusa kumativuta pompano brother wake wa munthu ameneyu wativuta ngati kwambiri kupha anthu osalakwa ,chauta wamutenga ,brother kufuna kutenga boma mwakuba, zakanika apo mukamuvoteranso,umbuli umenewu udzatha liti? kulemerako adzingolemera okha basi pano ndi izo ivutika ndi nomwenu kaya zanu komko