Email a copy of 'Chakwera walks last born daughter down the aisle' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

50 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
ngerengere
ngerengere
8 years ago

no parent wishes his children to misbehave and to attack other leaders just becoz yours is married is useless what if she were married to Obama mukanatukwana mtembo unfortunatel ndi mavenda azanthu omwewa and she is not the best out there

Tione
Tione
8 years ago

Musayambe kumunamizira Malryn che Nathan. Ngati mumamufuna mukanangonena kuti mwachedwa kufunsira. Mumachedwa ndi bowa bwanga. Wapita basi ngakhale munene zofuna kusokoneza zakuvutani.

peter
peter
8 years ago

Watichotsa manyazi tonse akhirisitu zikadakhala kuipa tonse tikadachita manyazi ‘pajatu amati ikaola imodzi zaolazonse’ Thank You Dr. Rev

tewete
tewete
8 years ago

Zauchitsiru izi basi.Dont say Munthu wa Mulungu coz adathetsa ubale ndi Mulungu.

Mungawa
Mungawa
8 years ago

my friend, dont wary. It happens kwa an2 ambiri so just 4get her and start new lyf. Let her stay peacefully in her just wedded family. Be a man please!!!! Dont curse her ever bt wish her good things

Nathan
8 years ago

Aaaa Malryn, wakwatiwadi iwe, ine kundisiya pa dzuwa! Paja tinapangana kuti tikwatirana pa 25 December tu! Poti tsopano ndiwe mwana wa Purenzidenti wa MCP ndi mtsogoleri wa Otsutsa Boma basi wayamba kundigenda ndi miyala!

MOG
MOG
8 years ago

Za ukwati zomwezi, zokamba, “mbweee!” Manyazinso mulibe. Kaduka basi. Mukhalira zomwezo, anzanu akupita patsogolo.

Bravo
Bravo
8 years ago

well done chakwera we adore u

box13 bilila NU
8 years ago

None of our business, ma ukwati ena anachita tsiku limeneli osalemba pa nyasapa bwanji ?za ziiii anthu akukwatilana everyday, m’ma midzimu.

Cash Gate
8 years ago

kulera kwabwino, congrats

Read previous post:
Malawians being short-changed

When people are desperately in need of something, they usually refer to a statement which says that half a loaf...

Close