Email a copy of 'Chaponda elected chairperson of AU Ministerial Panel' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Chaponda elected chairperson of AU Ministerial Panel' to a friend
Malawi Congress Party (MCP) president, Lazarus Chakwera, who is also leader of opposition in parliament. Is on a political tour...
Hastings Banda under MCP,led the nation into political devide by introducing the satanic QUATA SYSTEM followed by brutal repartriation of Northerners from South and Central Malawi.The arrival of Bakili Muluzi,seemed to have slowed down the tribalistic momentum.Kudos to Bakili Muluzi for his undaunting partriotism which held our nation together for at least a while.His unthinking judgement to campaign for an evil rogue Bingu Muthalika,has indeed,catapulted our nation into a political quagmire which if left unchallenged,can easily turn our beloved Malawi in to a sea of hell.The leader we are seeing to day,Peter Muthalika,is part of a conspiracy theory.By grooming his… Read more »
Zoonadi,ndatha kumva,kuona komaso to forsee kuti a Dr Chaponda is be GROOMED to be NEXT PRESIDENT in 2019
Chilima,aziwonere yekha pamwambi wakut,ndiwolotsa ndikakutafune
Ngati pali mbutuma ya munthu ndiye George chaponda. ….why are you people just benching a capable person like Saulos chilima? Here’s a tried and tested multi million dollar company CEO and all you can do is send him to watch Magufulis inauguration. …the important things you send Honourable Ziphwisi law? Shaa!
In the land of Mulhako utopia, no citizen thinks they will be ruled by other tribes again!
DPP, please start to think National and not Mulhako all the time!
Kodi chipani cha DPP ndi cha a Lhomwe okha?
Saulos Chilima should have been the rightful person delegated to this SUMMIT. The writing is on the wall we all can see it.
observer@ 3, uzimva chizungu. ‘elected’ ndiye kuti panali chisankho, wina ndikupambana. ‘appointed’ ndiye kuti angokuwuwuza kuti ukhale apa. nyo!
Some of the agenda items have hit Malawi hard ndiye inu ngati chair mudziti chiyani zakwanu? Sound leadership?
A new president a dpp, osatenga bright msaka bwa. Koma iwe uletsa anthu kuphwisawe eti
malawians on the world map. uku omwayi kumwenda otsala pang’ono kuti owine zawo zija, uko obushiri okudya vindalama zedi, kwinako ogolden boy okupanda azungu daily, otay grin ndiye awo okungoyimba vinyimbo vabwino vokha-vokha mpaka kulandila navo ulemu ku mangalande, nanga mkwazi uja documentary yake idawina mpikisano uja bwa?…zikuyendatu ati? osayamika apa ndiodjwala chabe.