Email a copy of 'Charis Missionary Church endorses Mutharika for 2019 Malawi elections' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

35 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
Vindere
Vindere
5 years ago

Born and raised in Mzuzu never heard of this Church, where exactly is it

Bristone Mabichi
Bristone Mabichi
5 years ago

Pepani abale ndi alongo walankhula’yu ndi munthu ngati inu nomwe, chonde musachimwe. Komanso iwe Eleck Phiri, samala chifukwa uzalakwitsa nkhosa. Komabe, mpoto yiti yatukuka? Mukalandira ndalama muzingoti zikomo kwa amene wakupatsani osanena zambiri. Mulakwisa ambiri. Kodi mumatha kusiyanitsa ntchito za boma ndi munthu woyendetsa boma’yo? Boma liyenera kutukula dziko lonse mosakondera. Iweyo ukayang’ana ukuwona bwanji pa nkhani ya chitukuko m’dziko lino. Siya chibwana.

Central
Central
5 years ago

This is Malawi’s Judas Iscariot, kupeleka ana a Malawi ku mikango chifukwa cha ndalama, my foooooooooooooooot!!

Kukoma kwake Mulungu anatichenjeza kale kuti si onse amene akutinamiza panowa omwe ndi ake enieni………….. enawa ndi ma church a chipani, mulungu wao ali kuchipani konkooooooooooooooooooooo kuteloko Erick Phiri uku mwina ndi disciple wa mtsogoleli ameneyooooooooooooooooooooooooooooooooo ndiye akufuna kupusitsa ndani? Waupondaaaaaaaaaaaaaa Phiri wamvaaaaaaaaaaaaaaaa!

mtete
mtete
5 years ago

QUOTA system is here to stay. Any presidential candidate fooling people that he/she will abolish the system is lying.

Ever wondered why APM, Chakwera, SKC and JB scarcely dwell on the issue? It’s because Malawians like the system.

Themba Mwambira
5 years ago

Anakuyitanani ku Mzuzu State Lodge?? It’s the Government responsibility to bring development to every part of the country because they are in charge of our TAXES and all donor money. This doesn’t warrant them to continue ruling thus country in any way….. Inu pitilizani kulalikira Za uthenga wabwino wa Yesu Mkhristu. Zovota aliyense adzagona yekha osati kutsatira zonena inu ayi.

Wahy
Wahy
5 years ago

Okay nanga why did other governments fail to bring development to the Dead North?

JAFALI
JAFALI
5 years ago

THE PASTOR ELEKI PHIRI IS A BROTHER
TO THE LATE DANIEL PHIRI —

Alamu Pumani Mwakula kuba

Dpp is slowly killing the north through the quota system of education. You work hard for nothing in schools. Names like Mkandawire, Gondwe, Nyirenda, Chirea and Mwas are the most vulnerable. Mark my words. Bandas, Phiris, etc can lie should districts of origin to run away from the harsh hand of dpp Lomwes. Mungamasekerere mseu basi. Stupid. Education is development that lasts forever. Stupid church.

mada
mada
5 years ago

ndalama za Achimwene ako ulinazo ndi zakozomwe komaso za 5 years ukumaliza pa 2019 ulinazoso tazisiyeni izi zikubweleselani bp

flose
flose
5 years ago

huwu siufumu bambo 2019 mutulukamo mboma Achimwene anu 10 years inuyo 5 years mukufuna mukaleso 5 years ina banja lake lomweli , zatitopesa tione zina bambo , mwakulaso siziyenda mboma moso

Napoleon muza
5 years ago

You don’t have to be known to say the truth. If you read the bible some are mentioned once but brought big changes to others. God can you anything to speak for him. Remember when he used a donkey to rebuke a prophet? Remember when Jesus said he can command the stones to worship God. Read the story of Saul before he became Paul who turned baptised him after being hit by the light on the way to Damascus. So you want it to come from the big names to be true? Heheheh, read of people who were thought to… Read more »

Read previous post:
Sparc Systems growth attracts American Company  NetApp

NetApp has disclosed that it awarded Sparc Systems with an award of the Fastest Growing Partner of the Year Award...

Close