Email a copy of 'Chewa Heritage disown arrested Gulewamkulu: Accuses Muslims of impersonating' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

41 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
Concerned Zambian
Concerned Zambian
8 years ago

Its good to read what people are saying about the issue. First and foremost everyone must realise that we all one people. We may belong to different tribes or religions and yet we are one people – whether in Malawi, Zambia, Mozambique or other country. whenever a problem has arisen, ensure you concentrate on the main ingredients and not the matters that might simply anger others. For example, do not mention the tribe or religion of those that were involved in the confusion and harassment of innocent people. Just allow the law to take its course. We live in a… Read more »

youna
youna
8 years ago

Gulewamkulu wa ku town amapangidwa ndi mijomba thats why amakhala wachisawawa. Eni ake a gulefe sitingapange utsiru ngati umenewu. Nyau za jando ndi zimene zikusokoneza. Munamvako kudambo kukumveka maina oti “Hussein kapena Issa”? Achawa inu chonde chonde leave gulewamkulu for the Chewas!! Mukakamira muzingoyaluka nazo…..

Kadziotche
Kadziotche
8 years ago

Anthu amenewo ndi agule basi.Kaya kwao nku Zomba,Mangochi,oro Ntcheu.Bwanji simukana pometa athu kuti nza a Chewa okha okha? Vuto la open access to culture ndi limeneli.Mpaka mzungu (ati a Chisale,wansembe wa Katolika) anameta ku Mua,ku Mtakataka!Kufwala gule.Nyau is an esoteric tradition koma inu wautchipitsa mwambo uja. Inu a CHEFO mwachepa.Mumangotha kutolera ndalama zopitira ku Zambia kwa Gawa basi. Milandu ikagwa nthawi zonse mumangoti “si ife”. Si inudi.Inu mulibe dabwe.Inu si mfumu.Mafumu anu mu CHEFOmo ali patali ndi pa ground pomwe pakuchitika zinthu.Chalo Lukwa,Chalo Kaomba ali ku Kasungu,mlandu wachitika ku Lilongwe ayankhapo bwanji? Ayankhe aku LL omwewo. Free advice: CHEFO should… Read more »

Kanyimbi
Kanyimbi
8 years ago

Hahahah, chilombo chogwira mabere a azimayi. Koma zilombo zinazi.

kate
kate
8 years ago

Musalire apa za gule wankulu. This is a demonic dance and therefore anyone associated with it falls under the same influence of demons.

magenge
magenge
8 years ago

Kodi achewa mumakananso abale anu. Nonse ndi achewa basi nanga ku Zomba mtundu wao ndi chani? Munthu kukhala Isa Hasan ndekuti simchewa? Mesa bola amake ali a chewa basi. Sir name sinkhani pachikhalidwe cha achewa. Za achewa izi ndi abale awo opanda mtundu. Two tribes are well known in Malawi Tumbuka and Chewa well maybe Yaos too the rest are covered under major tribes. Ngakhale Bingu anayesela kutchukisa muthako wa alomwe but most lomwe cannot even speak their language and pravtice Chewa language and culture

kk
kk
8 years ago

Muslims are not Yaos and Yaos are not muslims. Umbuli ku Malawi too much. Ena amati amwenye achiyao meaning amwenye a chisilamu.

2016 welcome
2016 welcome
8 years ago

Truth pains. Yes! Not all Yaos are Muslims but most Muslims in Malawi are Yaos. Fact. Again the same principle holds true: not all Muslims are terrorists but most terrorists are Muslims.

Saphwetha.
8 years ago

Islam isnt Yao and Yao isnt Islam,i know plenty yao christians,how does chefa knw if those guys are giving fakes names and home of origin if one of the guys is from ntcheu then probe these guys more.We have criminal minded pipo across all religions.

AKA NYAKWAWA
8 years ago

each creature in a mask isn’t gule wamkulj…..gulewamkulu is a traditional dance for the chewa which appears occasionally eg chizangala, maliro,ufumu and during political and many other developmental social gatherings…however….thieves, killers and other immoral pipo have taken advantage of the mask of gule wamkulu and would like to dent its immage…its defamatory to the greatest traditional practice for the chewa when some pipo use it in their own way…the gule wamkulu does not just come out without authority…when investigating this the police must ask who in terms pf a chief authorised the outing of the big dance…if it lacks backing… Read more »

Read previous post:
Kachaje on Malawi economy: What is our excuse?

In one meeting which I attended, a question was asked; “What should Malawi stop doing to make economic progress?” One...

Close