Email a copy of 'Chief Mwalweni of Rumphi campaigns for DPP in total defiance of electoral laws' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

23 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
Mike
5 years ago

Mfumu ya Chitumbuka. itavala duku ngati namfedwa. Eshhh kumpoto ziliko

UTM ref
UTM ref
5 years ago

DPP boma

Favour of Yahweh
5 years ago

Mafumu openya awa akudziwa zombie boma lawapangira, simungawatseke pakamwa ai. True has to be told. Mafumu amaona zombie zikuchitika, osati Isi mungotsusa koma simukuona ai. Keep up Senior Chief, afootokozereni anthu chilungamo, you sherperd them.

julius phiri
julius phiri
5 years ago

As expected, MEC will be clueless on how to handle this matter. Remember DPP has 5 Commissioners in MEC, they cannot bite the hand that feeds them . The commissioners will bury their ugly faces in the sand and pretend nothing happened.
What a shame!

Ndata Albino Auction Floor

These chiefs are intimidated by the government officials. They are forced to do things against their conscience. It’s all because of poverty. Poverty is the root of all the evil. Poverty drives people into criminal activities. Poverty drives women inti prostitution. Poverty breaks marriages. Poverty takes Uladi Mussa to different parties. Poverty is keeping Ntaba in dpp. Poverty is evil.

Favour of Yahweh
5 years ago

Nanunso chilichonse intimidation by government. Munthu asanene za kukhosi, asanene chilungamo waopysedwa ndi boma. Inu akukuopyesani osutsa boma. Let the chief help his people to do right thing, osati chifukwa inu milk ndi kanduka ndiye munyoze a mafumu.

Wilson
Wilson
5 years ago

Nothing will happen to this defiant traditional leader. Koma akanapanga endorse an opposition figure eg Dr Laz Chakwera, Saulosi Claus Chilima, pompo-pompo akanagwidwa ndipo tonse tikanati MEC inachenjeza za izi. MEC will be toothless on those glorifying the ruling elite. Search me

Favour of Yahweh
5 years ago
Reply to  Wilson

A Wilson, tamangodyani basi inu muzawatani mafumu world, ndiye kuopsezako kumeneko. Inu mukawakhazike pansi a mfumu, mwakulira kuti inu.

ANALYST
ANALYST
5 years ago

Malawi Electoral Commission ili pheeeee! Anayamba ndi uyu wa ku Chikwawa Lundu, pano ndi uyu Mwalweni! Demeti

HengaBay
HengaBay
5 years ago
Reply to  ANALYST

Tsono MEC itani ndi a galatiya opusa ndi aneneri onyenga amati mvotereni lazaro aja?

COPS
COPS
5 years ago

Kkkkkkkkkkkkkk kuwaona a Mwalweni wo iiiiii atichimwitsapo iyaaaaa……………….

Bristone Mabichi
Bristone Mabichi
5 years ago

KAPILIKONI mwenecho, utijiwonere wekha pala dazi lafika, 21/5. Lyaninge vyanthontho, ulunji wasuzga.

Vinjenje
Vinjenje
5 years ago

He is a stupid chief.

Favour of Yahweh
5 years ago
Reply to  Vinjenje

He can not be stupid because he has mind his views known. This is democracy, we differ, but that does not make you stupid, mukuyenera kulandira mwambo a vinjenje, manga mwa dzina Kanu. Mukufunika mupite kudambwe, kapena kuti ba, kundagala mukaphunzire chikhalidwe. Sititukwana mafumu chifukwa tasiyana Nasongole maganizo.

I shall be honest with u.

Afumuwo ndambwiyako?? M’mene atukwanila Lundu pamsokhano iwe ukuyembekeza kuti anthu asamuyakhe?? Ndindani iye simunthu?? Ayakhidwa basi kaya ndi azigogo ako izo ndizako

Read previous post:
Malawi govt hails Pope Francis, partners for donations to relieve flood victims

Minister of Information and Communications Technology Henry Mussa has  said government is  pleased with head of the influential Roman Catholic...

Close