Email a copy of 'Chikwawa Catholic priests donate K1million to flood survivors' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Chikwawa Catholic priests donate K1million to flood survivors' to a friend
The catholic congregation has pledged to donate to families affected by floods, all the money that will be collected on...
apa pokha ndikuti chauta alemekezeke komaso adalitse atsogoleli amipingo yomwe yatengapo mbali yothandiza azibale anthu omwe akuvutika chifukwa cha madzi osefukila
way to go Fr Jambo and Fr Semba. continue the commendable job
Good Samaritans
love of neighbour
A friend in need is a friend indeed……..
Proud of you dear priests
Catholics have assisted, nanga matchalitchi enanu mukuti bwanji? makamaka,mapente muchitepo kanthu. Tiyeni tonse tigwilane manja, imeneyi ndi ntchito yofunika makamaka pa nthawi ino pamene anzathu akusowa pokhala. Komanso nanu musamukeko kumeneko, mupita ndi madzi nonse ngati simusamuka.
Zoona, inu mapente odziwa baibulonu, Abusa anu ntchito Yao is to give ma account number awo pa mapemphero and pa TV for donations why not show now that you know the bible which teaches the greatest commandment is the one of love of both God and neighbor. Do you only love the people when they fatten your accounts through your threatening sermons? The only bible passages you know are the ones that speak about giving to pastors. Shame on you self annointed prophets, senior prophets, evangelists eats
thanks for good job God be with you.
our self proclaimed prophets can’t do this because they are satanists
Ndikuti kodi a jehova ‘s witness ( amboni ) alipo ?
Tikudikira kuti inunso timbveko kuti mwaperekako , kodi inu kwanu ndikulandila basi ? Tsopano lero ndazindikira kuti kamuzu sanalakwe kuwathamangitsa anganya amenewa .
Olo mutanditira doom sindingalowe mpingo umenewu . FULL STOP