Email a copy of 'Chiukepo inspires Nyasa BB win against Epac:  Malawi TNM Super League' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

9 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
KWEENI MPULOFETALE
KWEENI MPULOFETALE
7 years ago

Nyasa dubious penalties Ulesi…kukhalira kubelekedwa basi…

KHETSO SANAMA AYI
KHETSO SANAMA AYI
7 years ago

LINDANI MADZI APITE. CHAKA CHINO NDI CHA NYERERE BASI. TIDAKUTURUKIRANI. MUMADALIRA A REF KUTI AKUPATSENI PENALTY. If BB fails to score a genuine goal, the ref is ready to come to their rescue. How many free penalties have you been offered? Ingotini phee muwone. Chaka chino muwona bwadza. Sindidazione adachezera ndi kuziona.

markmarc
7 years ago

ndichifukwa Chake Feremuzi siichita bwino,aChiukepo zimawanyera kuchinya ku Theba lero asanduka dolo pa nyasalande!Malawi wanga uneeee

Cosmas kulugomba
Cosmas kulugomba
7 years ago

Maulee ndi maulee basi

Nganali kombweke
7 years ago

Ana achepa. Maule ndi more!

Emily Juma
Emily Juma
7 years ago

Well done Maule.Mwatimvetsa kukoma. Pitilizani kupambana ndipo timakunyandirani. Kaya zivute or zisavute tili pambuyo panu basi NGANGANGA.Kuno ku Phalombe

opportunist
opportunist
7 years ago

Ndiyo yake a Headmaster STD 3B i like that

Andrew Msichili
Andrew Msichili
7 years ago

Maule Kupitiliza Pomwe Tinasiila,blue Eagles Fans Take Care ,we Are Coming To Take Our Bag Of Money.Ndizandalama Izi.Sitinalowe Mu League Kudzasewela Kapena Kudzacheza

AV wa Maule
AV wa Maule
7 years ago

Koma luso loti Ukachinya iweyo anzako asachinyeso nde zopusazo. Ngati ndi zithumwa ukabwenze,luso ulinalo kale.

Read previous post:
People stealing church offerings should face  arrest – Bishop Mtumbuka

Bishop for Karonga Diocese of the Catholic Church Martin Mtumbuka has said people who steal church offering of plunder church’s...

Close