Email a copy of 'Civi society fear Malawi sliding back to ‘dark era’: Condemn ‘secrecy and lies’ President Mutharika’s health' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

12 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
LAZALO YONA
LAZALO YONA
7 years ago

Crazy drammatists in Malawi. When has it started for organisations registered to fight for minority rights to fight for the majority???/ Pali nzeru??? 2019 wooooooooh munya

Gringo
Gringo
7 years ago

Malawi has always been darkness, maybe it’s getting darker now.

patrick
patrick
7 years ago

Tatopa ndi ma blackouts, only high density areas alee ndi ma blackout, ku lilongwe area 10,12, ndi 43 alibe ma blackout, dont forget mazungu wa area10,12 ndi 43 samavota, anthu ama vota ndi ku high density areas

Phyuta
Phyuta
7 years ago

Sembereka khala chete ndi mano ako obvundao !!

OMEX70
OMEX70
7 years ago

Thumb up CHRR and CEDEP. for speaking the truth on this issue. You are only trusted COSs except on the issue of Same sex marriages. Mwakasungula and Billy Banda of Malawi watch have now become Government worshippers.

be humane
be humane
7 years ago

hypocrites, you let Billy Mayaya alone in the streets when you were planning the Demos together. Since his arrest mukuyankhula lero? Where were you all these days? Anthu oyipa inu adyera

Mjomba
Mjomba
7 years ago

Anthu inu ndinu zitsiru kwambiri, mmalo moti mukhale mkumakambilana kuti madzi, magetsi ndi njala tithetsa bwanji, muli busy kukambilana za moyo wa munthu, mukuganiza kuti tikusankhani kuti mukhale President, abusa a Sembeleka bwanji osagwira kolona ndikumapephelera xa mavuto amziko muno kusiyana ndikumayang`ana kuti uyu lero wadzuka bwanji. palibetu chitukuko pa zomwe mukuchedwa kukambilana, atafa Bingu, mai wathu Joyce Banda analowa pa mpando kwa 2 years and inuyo a Sembeleka munali nawo pa chiongole, chomwe chidasintha mmalawi muno ndichiyani. Malawi sidzatukuka chifukwa cha nathu ngati inuyo. tiyeni tikambilane zamavuto okhadza aliyense mmalawi muno osati za munthu mmodzi, anthu akufa ndi njala,… Read more »

Chindere chakufikapo
7 years ago
Reply to  Mjomba

Kkkkkkkkk uyu nde chindere chakufikapo. I Thought president is a public figure aliyense ayenera kudziwa za umoyo wake pa Malawi pano. Chobisira utenda wa mtsogoleri wa dziko chiani? M;malawi ngati pali mbuli yamunthu ndiye ndi mjombayu.Workup mjomba we are in democracy.

LAZALO YONA
LAZALO YONA
7 years ago

Idiot. Akakhala ku parliament president wanu ndi Lazalo koma akangopita ku US ndiye mukumusandusa kukhala president wanu. Iwedi ndi Chindere chenicheni.

Samatero
Samatero
7 years ago
Reply to  Mjomba

The president is a public figure that’s why we need to know. We don’t want to hear about Sembereka, who is he to the nation of Malawi

Mndambala Boy
Mndambala Boy
7 years ago

Bwanji nanu ngati zopanga demo zimakukhudzani simumapanga nao?bwanji inuyo simunapiteko? zopusa basi!!! asha koka inu!!!!!!

Opals
Opals
7 years ago

Thumbs up for calling out this untowardness. These DPP fellas forget they are not in power by entitlement. Let the Rule of law not of man prevail. They should exercise power reverently coz they occupy positions of trust. Malawi is for all it’s citizens.

Read previous post:
Are Malawi insurance companies starving amidst plenty?

Malawi’s economic and marketplace developments suggest a continuation of challenging and highly competitive conditions for the country’s small but growing...

Close