Email a copy of 'Controversy surrounds North Malawi League, fears of match fixing' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

15 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
Namachinda
Namachinda
9 years ago

Northerners,every season wararawarara eeish.Mpira simutha ntchito kugawa mapoints mu super league basi m’malo moti muzilimbikira kumpoto kukhale matimu olo 4 mu TNM ntchito kukokana eee federation eee Nyikaland.Nanga kupanda Moyale kumalimbikira bwino kulibe team kumpototu

Roots
Roots
9 years ago

Why is it that our colleagues from the Northern League fail to be demonstrate professionalism? If your failing to manage a small league like Simama, how about taking the leadership? Muzazitha inu? Your collegues from the Chipiku nad Nsenjere have identified the promoted team kom ainuu year in and out mlandu basi..Utumbuka eti

Martin
Martin
9 years ago

Palibe kugwirizana pakati pa mpira ndi federation.Mukungosonyeza umbuli wanu abale inu.Sukulu ndiyofunika.Federation izachitika,mufune or musafune,Mbuzi Inu

Mbunama victor
9 years ago
Reply to  Martin

even in parliament akumamenya anthu ogwira ntchito ,nkhanza too much how can they rule since they have shown the world their disorganisation in simple things & they can not be trusted with bigger things

Suicide Bonza
Suicide Bonza
9 years ago

Always Mzuni is on loosing side though amakhala ndi valid reason

Citizen
9 years ago

Koma Kumeneko North Woyee!

chefourpence
9 years ago

atumbuka! Eish!

Daniel Phiri
Daniel Phiri
9 years ago

Still, Federation is the only answer. Then we can have our good sons who are at FAM come home and help run things.

Ine chiphwisi chaku barracks komwe ku Wings

Kodi zantchito mwaiwala mwasanduka a mpira? Tikhale ndi matimu angati mu super league? Bwanji ndalama zimapita ku mpirazo mutakonzetsera manyumba akukhalira kuukhawa. Two or three military teams ndizomwe tikufuna osati mpaka akwane six aaaaaayi zikumatichititsa manyazi. RSADF munaimvapo mu ABSA league? NRFAL sakulakwisa nawo zawakwana. Nanu a FAM chitaniponi kanthu mwa nsanga super league isanasanduke MDF league

Tawonga
Tawonga
9 years ago

Koma kumeneko ku nyikaland. Nanga mukazakhala panokha ndiye eshiii zizakhalakotu.

bbsupporter
bbsupporter
9 years ago

Anthuwa ndi mbuzi zenizeni,samadziwa kuyendetsa mpira achoke.

Read previous post:
Malawi seeded in Cosafa Cup set for May

Malawi national football team, the Flames will be seeded from the preliminary round of the 2015 Cosafa Cup due to...

Close