Email a copy of 'Court dismisses judicial review on UTM registration: Lawyer Bob Chimkango ‘frivolous’ application thrown out' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Court dismisses judicial review on UTM registration: Lawyer Bob Chimkango ‘frivolous’ application thrown out' to a friend
Key media houses in Southern Africa continue to be awash with extensive coverage of Prophet Shepherd Bushiri’s launch of his...
This is abuse of court process allow the registration of UTM and do not block it. We are in multiparty democracy but DPP want to take us aback. APM was not there when we were voting for this democracy and please don’t spoil.
Even DPP itself is flavorous, vexatious and hopeless. Anthu osamva!
Komatu abale azizi akupanga si a DPP koma a MCP. Mundikhulupilire ndithu, umboni ndiri nawo. Team MCP siimafuniratu UTM ati chifukwa ndi team b ya DPP komanso ipatula ena mwa mavoti a MCP. Musade DPP siikutekeseka ndi bus company, amene akubvulala kwambiri ndi a MCP.
Retard lawyer now appointed Company Secretary. This Bob has failed miserably to run his own firm and boot licks DPP kuti awonekeko pa town otherwise he is a fucking useless citizen. Hule lachabechabe
koma ndiye mwalimbana naye uja mumati babe………….UTM/SKC moto kuti buuuuuuu 2019 boma
…….’frivolous, vexatious and hopeless’….. koma apumbwa muli ndi khama osangozitaya bwanji
Musamalimbane naye chilima mukuva kuwawa
Well written brief news item there Wongani Chiuta. Many out there do not accurately report court proceedings.
A Mike Tembwe kumaiona game ngati ma lawyer onse m’Malawi muno akungolozera kwa UTM musamaletu ndi MCP yanuyo a Chakwera chiyambireni campaign anadzangodutsa ku Zalewa mpaka ku Mwanza & reverse osaoloka Shire waku LL via lakeshore road ndiye kudziwa campaign kumeneko, anthu ali mu BT koma a Chakwera kumangolambalala eeish!
Mcp kkkkkkk vuto la a Malawi sitichedwa kuiwala
How can anyone fully grown person vote for DPP?
Simply because he is a grown man. Ana onse aku mkaka, osakhwima pamchombo, obvala thewera apite akavotere mwana nzawo khanda baby chilima. Omatenga anthu azipani zina kumawapatsa ndalama kumawalankhulitsa pamisonkhano yake nkumati ajowina. Ndichifukwa chake anthuwo akumayankhula poyera kuti abwera kudzagwira ntchito ya malawi congress party pa msonkhano wachilima.