Email a copy of 'Court ruling gives leeway for MCP convention: Kaliwo, Msowoya’s suspension upheld' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Court ruling gives leeway for MCP convention: Kaliwo, Msowoya’s suspension upheld' to a friend
Former Vice Presudent Dr Justin Chimera Malewezi has given his views on age-matters debate following calls in ruling Democratic Progressive Party...
kkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkk msowoya and Kaliwo are corrupt leaders that malawians do not want to see their faces or hear their voices. they got bribes from DPP together with Kabwila so that they can disorganise MCP! You idiots you have failed big time!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!
Odi uko, Kaliwo & Nsowoya chondeeeeeeeeeeee patukani a bwana adutse nawooooooooo………………………………!!
MCP NGC changu changu convention ichitike pomanopompano……………………………………………………………….!! Chiswe chodula m’mera chadya misinde yotchedwa Nsowoya ndi kaliwo……………………………….. koma kumeneko, moto kuti buuuuuuuuuuuuuuuuuuuuuuuuuuuu wina walira ngati mwana amvekera nayekaaaaaaaaaaaaaaa
Looking forward to a
Successful / prosperous convention
–Don’t let malawians down !!
All Kaliwo wanted was to use Msowoya as a pony for tax evasion on the car that he had imported, he is a man with no morals.
No sensible MCP member can vote for Kaliwo and his crooked boss Msowoya after what they have taken MCP thru….
MCP should move quickly to call for a convention and get rid of these DPP mercenaries and start preparing for the general election with full momentum .
Let Msowoya shallow his pride and apologise or let him go back to him now heavily divided DPP party.
Kanthu ako. Munthuyi atenga u President poyela yela ndiiiiithu
tiyeni nazo , chakwera moto 2019 boma. WINA AFUNE ASAFUNE CHAKWERA NDI BOMA BASI!!!!!!!!!!!!!!
Enanu ndiye mumati chiyani. Ife tikupakira katundu wa ku konveshoni ku Mzuzu. Enanu tiyenayoni miseche yanuyo yokhudza kamwana kanuko.
Pamene a MCP akutuluka m’bwalo la court, tipemphana kuti a DPP akomzeke
Akaliwo ndi asowoya muli mmadzi,omwe amakutumani kuti msokoneze Mcp, nawo Ku chipani kwao zasokonekela,alibenso nthawi yanu,nde tiwonana ku comvetion
Kaliwo wadziwa Bangwe see the placard carried by a lady in teeshirt ukabweze K 300, 000,000