Email a copy of 'Crack the whip on DPP members in civil service - CSOs' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

13 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
mjiba
mjiba
5 years ago

I miss the times of Secretary to the President and Cabinet, John Ngwiri, Kakhobwe, Mc Donald Banda, Justin Malewezi, Alfred Upindi men who knew what the Civil Service was all about not these madeyas who are made Chief Secretaries to OPC? My foot.

CIVIL SERVANT
CIVIL SERVANT
5 years ago

Some animals are more equal than others in this animal farm called Malawi.

ndele
ndele
5 years ago

malawi is 200 years bihind.cipwilikiti, kumbwambwaitsana the list is too long kwa ma agenda osayamba, olekezera panjila, opanda umboni, under the leadership ya DPP. SO monga ananenera mai dzimbili ndithu tamva kuti olo ku paliament ena akanena fundo zofuna zinthu zisinthe pamapezeka okana kusintha zinthu. so !!!!!!!!!!!!!!!! tikakusankhani ndi mmene mmatitaila kumphepete. tamva nao by the way nkhani ya chaja $75 visa is toatal ridiculasi. and then one pays 5 pin for another month over, and pssengers have paid k300 when exiting where does all this money go when we dont see any change in our airports please, ZOONA ku… Read more »

pathfinder
pathfinder
5 years ago

Guys get this in your thick mamina skulls. Anthu amene akuchotsedwa ntchitowa saakugwira ntchito zawo zomwe analemberedwa kuti agwire ndipo amene atsalawo ntchito zawo zikuoneka. Nchifukwa chake ambiri a inu simudzatukuka ngakhale kuyanba ma company chifukwa muzidzasunga anthu a ulesi komanso oukira mabwana awo kapena ma supervisor awo chifukwa cha nkhwizi komabe osawachita discipline kapena kuwachotsa ntchito even though you know its not good for the growth of the company. Mbuzi za anthu ngati Mtambo.

James
James
5 years ago
Reply to  pathfinder

Pathfinder, politics have made you dull. I used to give you respect sometime back but you are reduced to zero now. The law says civil servants MUST not be involved in active politics and no more. Please come back your senses.

pathfinder
pathfinder
5 years ago
Reply to  James

kkkkkkkk choka apa James ndidakali yemwe uja. Tsono inu mukufuna law idzigwira ntchito nthawi yokomela inu? Nthawi yonseyi achina calista asanachotsedwe bwanji simunayankhulepo kuti achoke kuntchito zaboma chifukwa ndi atsogoleri a UTM? ooh panopano achotsedwa ntchito mpamene mukufuna kuti law igwirepo ntchito chifukwa wachipani chanu wachotsedwa? By the way when is UTM convention? Better yet what happened pamene Chilima anakadandaula kwa judge ku high court zokhuza mpungwepungwe wolenbetsera chipani chake kwa olemba zipani? Kapena anaiwala kukaonekera kwa judge pokhala kuti analedzebwa ndi kachasu? kkkkkkk Koma chilima ndi otsatira ake, you guys are really a big joke.

LEGO
5 years ago
Reply to  pathfinder

You are so pathetic in your comments…Your comments are always contradicting with the views of most suffering Malawians..NO matter you love DDP but sometimes learn to understand the laws

mtete
5 years ago

Really Chief Secretary! Even a kindergarten knows Civil Servants should not engage in politics. Why, then, do you allow this to happen and why double standards. Should we say this is silent confirmation of breakdown of good governance? Who is making your work difficult?

#DzukaniAmalawi
#DzukaniAmalawi
5 years ago

Lloyd Muhara is a brave man by issuing the memo. Gift heads should take the memo seriously and fire all civil servants active in politics. Failing to do so would tantamount to insurbodination and therefore such officers will be charged for not acting on a lawful instruction. Let the game begin!!!!!!.

abiti
abiti
5 years ago

Inutu phuma awotu awachotsa kamba koto their services not needed 😂😂😂😂😂 while AG and the rest are still needed lol..mumva pheni

Mchacha the Terrorist
Mchacha the Terrorist
5 years ago
Reply to  abiti

@ abiti

Childish

Dipipi wa Yudiefu
Dipipi wa Yudiefu
5 years ago

This government is working as if it’s not headed by a professor of law. That is why a lot of people believe that he is not in control of issues in this country or he is simply a cabbage. Kupanga zinthu zochita kuwonekeratu kuti zikulakwikwa. Sikuyambitsa ndewu kumeneku, kumapanga anthu ena ngati sikwawo kuMalawi.

Nalingula
Nalingula
5 years ago

CSOs should Try as much as possible to be pro Active .As for the UTM members they should have Resigned -Penapake mukumatikayikisa zochitika bwanji. Anthu asiyanisa bwanji UTM ndi DPP ngati Nonse mutokakamirabe mboma uku mukuchita Ndale.

Read previous post:
Is the judiciary muzzling freedom of expression in Malawi?

UTM’s decision to challenge court injunction obtained by Muli Brothers and Others not to comment on the matter between Sunrise...

Close