Email a copy of 'Criminals gun down one man in Lilongwe' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

65 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
Suwed
9 years ago

Apolice koma kugwira wonyengana galimoto koma mbalaza mfuti kulemphera kuchita nazo……..shame on you?????

Stevovo
9 years ago

Akubawo amakhala atagwilizana kale ndi apolice pokaba.

Paul ziga Tembo
Paul ziga Tembo
9 years ago

Malawi is small county but leaders failed to control such stories but I blame the government are not put effort on security issues just magin a police station having only one car and is better everyone who is police officer must have gun osati ndodo

ruth warren
ruth warren
9 years ago

A question i struggle to answer kodi anthu akubawa amawaphunzitsa kuombera ndi ndani? Nanga Mfuti amazitenmga kuti? Who supply them with bullets? This is pathetic. Imagine mbava ximenexi zikuchita terrorize homes by coming in groups of about 50 per home, kudziyimbira dzapolisi osabwera wats wrong?

YOLANDA
YOLANDA
9 years ago

MINE IS A QUESTION KWA NONSE AMENE MUKUDZITCHA KUTI MBAVA,KODI BWANJI SIMUKUTHANA NDI ACHISEMBWERE OMWE AKUNGOYENDAYENDA MTAUNI USIKU KOMANSO KUGWIDWA?

MULUNGU AKUYENDERENI MWAPADERA.

Chindazi
Chindazi
9 years ago

Very Bad… RIP…

Policemen,,, what are you paid for….. ntchito kumanga mahule utsiku,,, later on kugwira galimoto yoti ilibe indicator….

Can all policemen, including traffic police be redeployed to provide security in the locations…. rather than kumalimbana,,, sunamange seat belt,,, mkazi oti ali ndi mimba,,,,mukuthamangisa galimoto over 50 lipilani 10pin,,,,, kusiya mbala zikupha anthu ngati izi……

luvolwethu mpeta
luvolwethu mpeta
9 years ago

nde wa polisi akawombera mbava inu amabungwe nde muziti nfweee nfweee nfweeee mbofyoooo mbofyoooo mbofyoooo???????????? do you now see what these animals are capable of doing???????????????????? these monsters do not deserve any sort of space in our society, lets wipe them all!!!!!!!!!!!!!!!!!!!

maframes
maframes
9 years ago

This is very unfortunate, it is had to believe what is happening. people being killed like dogs, where is Police?
I really don’t know if we are safe at all.

Kazani
Kazani
9 years ago

We need tight security in our country.

Ngongoliwa
Ngongoliwa
9 years ago

THIS IS THE SPIRIT ALL MALAWIANS MUST EMMULATE. PLEASE BOMA, HERE IS A REAL HERO, DO SOMETHING TO FAMILY MEMBERS OF THIS HERO AND MARK HIS GRAVE WITH DIGNITY OSATI ZOMALEMBA MAKHOMA A NDENDE PAMENE MUKUDZIWA CHENICHENI. MUSAIWALE MUNAUZA AMALAWI KUTI BINGU SANAMWALIRE MUKUCHITA MISONKHANO USIKU KUTI MULANDE BOMA MOSATSATA MALAMULO, ZANKUTU!!!!!. KUKOMERA KWAKE A MALAWI SANAKANGALIKE NDIDZAUTSIRUZO KAYA MUNAONA KAYA!

Read previous post:
MP Mwenifumbo bemoans intraparty democracy in Malawi

Karonga Central Constituency parliamentarian Frank Mwenifumbo has expressed his discontentment over the state of intraparty democracy in the country saying...

Close