Email a copy of 'CSO’s change demo route in Lilongwe, set for 'red' street protests' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'CSO’s change demo route in Lilongwe, set for 'red' street protests' to a friend
Malawi Congress Party (MCP) president and leader of opposition, Lazarous Chakwera has thanked Malawians for their comforting during the bereavement...
Kikkk, there were about 30 people at the LL demos
this is tribalistic and its against the Lhomwes
I hope this is a peacefull demo bcause some people they take it assive its an opportunity to rob peoples shops and cause havock in the city.Afterall which affects the economic activities going on.
Koma atumbuka, achewa, ayao, angonde, atonga, asena, amang’anja, etc etc ndife wopusa kwambiri tonsefe basi lomwe kumatilamulira? Komanso pachibale pachichimwene. Wamkulu kulamulira kenako wamng’ono mwina 2019 mwana wa Bingu or mwana wa Peter who knows?????????????
Ndiye titani? Basitu ma demo womwewotu mpaka 3030 kkkkkkkkkk
Bola azathu ayao analamulirako kawiri Muluzi and JB. Achewa at least ngakhale kamuzu anali wa fake komabe anatinamiza kuti anali wa kukasungu…………kkkkkkkkk
Nanga mitundu inayi makamaka mtundu wangawu Mtumbuka ine ayi ndithu ma demo basitu or else Federation/Secession no turning back kkkkkkkkkkkk
Among all the places for planned demos only Karonga in the north is not a city.If somebody says that north is being used as D 7 can we complain?
Non starter
MADEMO ACHITIKE. ZILIBE KANTHU KUTI BOMA LAKHALA MASIKU ANGATI. CHODZIWIKA NDI CHOFUNIKA NDIKUCHITA MADEMOWO MWA UFULU NDI MWAMTENDERE. OFUNA APITE, OSAFUNA AKHALE. MULUNGU ATSOGOLE MTUNDU WA A MALAWI. MTENDERE PATSOGOLO. LONG LIVE DEMOCRACY.
Even 10 people are enough to present the petition. So was the first lady right to get the money? Mulhako to hv the money as well? If u are happy about that then just keep quite. Amene mukuyankhula zachamba simunayambe mwapangako ma demo ever since
Ndikale lija ndivala red red throught. Mmawa kuli kanthu!
Tipanga mawa apo bi wina amwalira