Email a copy of 'CSOs demand probe into death of Judge Bakuwa in Zambia over ‘maizegate’: Dausi says idea pooh-poohed' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'CSOs demand probe into death of Judge Bakuwa in Zambia over ‘maizegate’: Dausi says idea pooh-poohed' to a friend
Minister of Information and Communications Technologies Nicholas Dausi has disclosed that the Public Service Reform Commission (PSRC) functions have reverted to the Office...
Koma inu acimwene ndakondwa nazo momwe mukulankulila. Anthuwa ndi atambala omwe sakafuna kuti judge uyu aulule zomwe ankachita ncifukwa chance anamupa. Siyani achite investigate mukaone zikatulukemo
I guess Bakuwa might have died in hospital. If his death certificate just reports natural death as is always the case in many hospitals, pathological examinations might be required to really establish his real cause of death.It may even involve exhuming his body for this process to take place.
Highly sophisticated saga as former zambia agric minister and state house are involved in this matter..
ambiliwa ndi ma machine tu. tiana mbwee, ndi zibwezi zowakakamila. kkkkkkkkkkk
abale 99% ya mabwanawa ali pa ma ARV nde kwinaku tingotengerako masoka kumafufuza mbili zao kuopa azikazawo angangogwa nkufaso kusiya maka zizukulu zomwe zikudya ma tax athu mwa kathithi. za anawo anamaliza kale ma skool.
anthuwa amayenda ndi zigulu( dzima botolo zikuluzikulu) olo zikwatu meaning maphukusi a ma ARV. abale simmaona nokha mmene anthu akuonekela matupi osafagawika bwinobwino.
zimimba, zipumi phuliphuli, milomo psuu, mawele kumamela mamuna wokhwima kale, tikati nkhope kukungika.
asatitayise nthawi.anadya zathu heavy nanga ali kuti nazo enawa azilondola mbwiyo muno.
So we should take it that Dausi knows something about the judge’s death hence his denial of investigating? We know Dausi kills people using his the NIB guys he used to kill Issah Njauju. We can’t rule out assasination here because this government has no room to accomodate dessenting views.
Good people where is Mabvuto Bamusi? Is he on holiday?
Not heard him talk recently.
Mavuto Bamusi has a stake of beef in his mouth, if he talks the voice may not be clear because he feels sweet. If UNIMA students intend to carry demonstrations, Bamusi will be the first person to ask the boys and girls to remain quiet because the government is looking into their issues. That is his duty in that office. That is Malawian life of survival, try yours.
kodi zakuti akulu akuluwa amayenda ndi matenda simudziwa? zibwana bwaanji? apangatu zambiri anthuwa
Iyi’tu iyi ndiyakusyawusya!
Nkhani njaikulu. Kuyendesa boma amai ndi abambo is serious business