Email a copy of 'CSO’s link electricity crisis to Malawi failed leadership: Call for 'Day of Rage'' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

9 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
Santana
6 years ago

Nzodziwikiratu kuti DPP yawononga Malawi. ESCOM ndi company ya boma a dpp amapita ku ESCOM kukatenga ndalama za campaign ngati momwe anachitira ndi Mzuzu city council and LWB and BT city council. Wina afune asafune boma MCP ikutenga come 2019. Tifuna anthu ofunira Malawi zabwino osati alomwe odzikonda okha. Anthu tikukhala mumdima wa ndiweyani a dpp akuti chimenecho ndiye chitukuko, cry my beloved country.

Jamax
Jamax
6 years ago

CSO’s in Malawi is but helpless and clueless believe me NO sensible Malawian can listen nor follow you now. You are like a crocodile without jaws – you like eating donors money by cheating them that you are fighting for the voiceless but when you recieve money you call people to the streets who are usually killed or wounded afterwards you escape to your mansions safely leaving the poor in cold blood.

Dzanjalimozi
Dzanjalimozi
6 years ago

Iiii komanso azibambo ma gay inu mukumatibowa tsopano. Mulibe chochita china? Nthawi yolimatu ino anthu azipita pa nsewu azikapanga chani? Tikakayenda magetsi abwera?? Kodi mukalemba ma proposal anu then kulandira ndalama kwa ma donor mumatiitana kuti tikapange march tikagawane dollar zo. Fotseki

mchawa
mchawa
6 years ago

olo iwe wa DPP kunyumba kwako kulibe magetsi lero

patrick
patrick
6 years ago

escom should employ foreign experts or privatise it, if it stays under government it is always prone to financial abuse and things will never improve

nyaxy
nyaxy
6 years ago

Iwe cloud ndi mphaso kodi amakutumani . ndindani? mkwuziwa nokha kuti ntchito za magetsi ziri Manja mwa Escom chochulirapo DPP ndichani ofunika kukufufuzani mmene mumakhonzera muli pa secondary level chifukwa zimene mumachita zimaonekeratu kuti osayamikira DPP angakhale kamodzi kokha munthu amathawa pa njingay mubvekere DPP aaa Muyalukanazo

Igwe
Igwe
6 years ago
Reply to  nyaxy

Olo chitsiru sichingayamikile DPP ndiye iwe nyaxy ukudabwitsa kuti mwina umadya mabi mutu wako suyenda

woman
6 years ago
Reply to  nyaxy

Nyaxy ndiwe munthu opusa kwambiri, kuwombera mmanja mfiti za DPP bwanji? Escom is totally under government if u don’t know, and panopa akutizunza, kupha, mabizinesi athu aima, tikusowa pogwira and you talk rubbish!!! A stupid fool, kapena umalemba utamwa midoli or you smoke whatever weed?

Pedegu
Pedegu
6 years ago
Reply to  nyaxy

These people are misguided, they are forgetting that this problem emanated due to lack of proper planning by our previous governments, if ever they have solutions why not engage government and share their suggestions? ?? I think we have a lot of people who are mentally unwell in this country.

Read previous post:
Judge faults ACB in DPP’s Wa Jeffrey K900mil compensation

High Court judge Charles Mkandawire  has  rebuked the  Anti-Corruption Bureau (ACB) for “not being serious” on matters of national interest...

Close