Email a copy of 'Daniel Mulomo drags MCP to court over polls' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

20 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
Mwana nsena
8 years ago

Ngati analephera ndikuzivotera yekha. Not worthy. Just sit down and accept the results. Old fashioned man. The only thing mr mlomo can do is to become a shadow khansala for 2019 elections. Munalepheretsa chipani. Asiyeni amzanu abweretse mzeru zina. MCP for new blood

Chifundo
Chifundo
8 years ago

Had it been apezako timavote tochepa koma olo,ayi zisiyeni zakukhotizo kkkk.

Alungwana
Alungwana
8 years ago

Umodzi, Kumvera, Kukhulupirika ndi Kusunga mwambo should talk to Mulomo as earlier as possible.

Zuze Chilombo Chammudzi
Zuze Chilombo Chammudzi
8 years ago

Why did he participate in the illegal pools? If he won , would he have sued. The challenge with the old guys is they always think of their posts as zamuyaya.

Tunthu
Tunthu
8 years ago

A Mlomo adalowa nawo mu mpikisanowu ndipo analuza ngakhale ndi voti imodzi osaipeza, ngati chisankho chidali chosayenela adaloweranji, ndipo palibe amene adawavotera ngakhale mmodzi out of 400 voters?, koma mkuluyu adaipitsitsatu, kodi atabweranso anthu ovotawo poti ndiwomwewo adzawavotera, mwaulemu angozisiya izi nthawi yawo adyerera ndi mnyamata wao uyu kamata amapangira limodzi madilu azisankho kusiya anthu anthu kumatemga mphwemphwa atagawira ndalama zotsatira zake mzimenezi, Kamata paja adamthamangitsa kale pampano wa Director of Elections – kapumeni bwino malume

vwapuwvapu
vwapuwvapu
8 years ago

Mulomo ukuyankhula ku khoti kkkkk.

Che Ngana
8 years ago

Ndichisankho Chanu Chomwenso Mwaberana Kkkkkkkkkkkkkkkkkkkk Atambala Akujomphana.Heeeeeee Koma Nyenwa!

Peter Mathanyula
8 years ago

The works of DPP

Mlomo
Mlomo
8 years ago

How was he ambushed when the party announced about the polls through a press conference 1 month b4 the polls.What is unconstitutional about the polls when the MCP constitution stipulates that the tenure of office bearers is 3 years and yet Mlomo held this position for 7 years.The Dude is just confused that he is out of mpando wonona (posters chipani ndi ma shadow).He is finished!

Galazinyake Mphande
Galazinyake Mphande
8 years ago

Alomo vetsetsani ndimene dziko limayendera inu osapanga protest mukhala ngaa muwukira

Read previous post:
Escom shun Kalondolondo meeting: Stakeholders furious

Electricity Supply Commission of Malawi ( ESCOM) shunned a kalondolondo interface electricity assessment meeting leaving different stakeholders furious and warned...

Close