Davido show in Malawi not taking place
Nigerian musician Davido is not coming for the launch of the Go Green Campaign in Malawi as earlier publicised, his manager has confirmed.
His manager Kamal Ajiboye, said the artist will not perform this weekend in Malawi as they had planned because the organisers needed more planning to do to hold such a concert.
Davido was billed to perform alongside a couple of Malawian artists including The Black Missionaries and Lucius Banda at Civo Stadium.
“Davido is no longer coming to Malawi,” said Ajiboye.
Ministry of energy, mines and natural resources lead consultant, Stephen Otieno also said the artist will not perform but they are discussing with his manager to have him later.
nothing new here,…he cant come ofcoz….
Mhuu,last time twas The Messenger,now its Davido. Ku Nyasaland kumeneko.
we knew davido wudnt b coming to malawi…
Malawi kukhumudwisa,,mmalo momapeza ana amene aphukila kumene pa music,kukayimba ndi davido mukutenga nkhalamba,,ife brackmissionalys,,lucius banda tinatopa nawo,,kodi nanga gwamba,dan lu,,mwanache,,grant C,majako,john T,,ndi ena achichepele ali kuti???,,plz promote young stars not magogo like soja,and missonaries,,tinatopa nawo
I knew this show was not going to work. Ife we have been UDF since time immemorial and very skilled for that matter. We have contributed immensely to the party. We understand Malawi’s media and entertainment industry and you know that. Yet you chose to work with this guy who failed in Kenya and you call him your strategist? Fine your strategist but what does he know about organizing shows? The moment i met this guy going to promote this show at a Christian radio station in Lilongwe is when i knew he doesn’t know what he is doing and… Read more »
Well done.
Abale kodi za Davido Concert zikugwilizana chani ndi Atupele. leave my President alone. Ndi dhilu and mukudana naye chifukwa he is principled. He is the only one who can save this nation from the economic turmoil we are in. Lets leave our personal problems and not politicise everything. UDF why do you want to reap where you did not sow? Just save yourselves from further embarassments and put your hse in order. why wash dirty linen in the public? anthu opanda nzeru inu.
Wawatu wawa,muthu uyu sizaboza ,ndangwilakonaye ntchito,simuthu oyamika olo pangono.stop ndithu sawerengera kuti wathandizako chani.chihana adatani,ulendotu inu umeneu. Mwana amaliladi nditulo lake lomwe.basi basi ungono ungono ulendo. Ngati akukanika ka go green nde ziko anakalitha.?chiwaya moto moto
Ine ndinanena kuti uyu ndi baby. Chipani for sale.. koma chatha ngati makatani
Koma kumupanga chipongwe Lucious zoona? ndiye ndi zoonadi kuti achina Jamieson, Josh, Fawzia Osman, Adam, Ngwira, ANdanga anaponya paliponse. abale Ndanga ali mbuuu kikikikii koma amandimvetsa chisoni mwamva. Or running mate mmmhhh sakununkha kanthu. Koma Lucious yekhayo ndiye samutha akunama. Chimene chija ndi chitsulo chanjanji. Soldier ndi survivor. ife tidzavotela Lucious ku convention ngati president lol