He is back!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!
Kanyimbi
9 years ago
Pakafa nyama agalu amachuluka.
Blessings Marenso
9 years ago
Pofera Knows The Truth
Yankho
9 years ago
Jegwee osadandaula bola iwe watenga Dedza Young Soccer to another level. Uli ndi zambiri zoti uchite mwina anthu sakudziwa bwino. Ngati ma Officials anayamba kuyerekedwa ataye tiye tilimbikire kuyendetsa chipani chanthu cha Malawi Congress party ndi nzeru zakozo MCP 2019 boma. Za mpira zitaye uko, taona timu ya ku Drdza ikuyendetsedwa ndi Atumbuka iwo akufuna Federal System koma ife sitilora team ndi ya Dedza. Nanga a Temboawauuza kuti iwe akuchotsa. Panopa a Tembo ndi wokwiya kwambiri ndi zimenezi. Team slogan yake ndi Kwacha ndipo tonse amene tiri ma Supporter ndife a Kwacha. Ndamva kuti a Tembo atuma President wathu wokendeka… Read more »
panganeni ndiwe osokoneza galu iwe sikwanutu kumeneko and jegwe pa easy agawe ma points amenewa basi mukuwona ngati ma gate collections muzidya angati muli ndi ma supporter ku bt inu akapamba well done coach.
BALITCHI baliman
9 years ago
Osadanda Jegwe, zinayamba ndi John Chilembwe izii.
He is back!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!
Pakafa nyama agalu amachuluka.
Pofera Knows The Truth
Jegwee osadandaula bola iwe watenga Dedza Young Soccer to another level. Uli ndi zambiri zoti uchite mwina anthu sakudziwa bwino. Ngati ma Officials anayamba kuyerekedwa ataye tiye tilimbikire kuyendetsa chipani chanthu cha Malawi Congress party ndi nzeru zakozo MCP 2019 boma. Za mpira zitaye uko, taona timu ya ku Drdza ikuyendetsedwa ndi Atumbuka iwo akufuna Federal System koma ife sitilora team ndi ya Dedza. Nanga a Temboawauuza kuti iwe akuchotsa. Panopa a Tembo ndi wokwiya kwambiri ndi zimenezi. Team slogan yake ndi Kwacha ndipo tonse amene tiri ma Supporter ndife a Kwacha. Ndamva kuti a Tembo atuma President wathu wokendeka… Read more »
Umbombo mwawona ngati mulemera nazo.
panganeni ndiwe osokoneza galu iwe sikwanutu kumeneko and jegwe pa easy agawe ma points amenewa basi mukuwona ngati ma gate collections muzidya angati muli ndi ma supporter ku bt inu akapamba well done coach.
Osadanda Jegwe, zinayamba ndi John Chilembwe izii.
Papa wangozolowera kutukwana basi umati asasiye ? Ndi ufulu wake u HSA sintchito?
mumutaya lero jegweyo?? poti wakuchotsan mmatope. plz my home district team dont do that.
Andrew bonya kaya mumati bunya wakondwano eti?sapesa zitsitsi ukuona ngati super league ndi chipiku eti?tiyenazoni