Email a copy of 'Defamation case: Nankhumwa, MBC want out-of-court settlement not Joyce Banda' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Defamation case: Nankhumwa, MBC want out-of-court settlement not Joyce Banda' to a friend
Malawi Congress Party (MCP) president, Lazarous Chakwera, who is also leader of the opposition in Parliament, on Friday toured Area 18...
kushosha bvumbwe opanda nkhuku, galu!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!
Nankhumwa wakhuta ndalama zimene anaba Bingu eti!!!!! Tionetsana, unali ndani iwe mimba kuno ndi uko chifukwa cha ndalama anaba Bingu…..Tamufunsa Pitalayo(Peter) kuti kodi ndalama anaba Bingu who are now the beneficiaries? Tikudzifuna ife akuba inu mwatichotsera Upkeep Allowance. shame mtundu wa Alomwe onse.
Iwe levelheaded, ukunama ma CCTV ku state house kulibee! Awa alomwe awa ali pa pressure ndi JB.
CHITCHETCHE CHOPUPULUMA ANAPHWINJA NDI MNCHIMBA MAN
I will follow in the wise words of the clever people,that says! In absence of the best,we anyone to fill the gap left by the best. In this case,its what happened with Nankhumwa,we all know he don,t deserve to be a Min of Information. But he got it coz of the following reasons,one coz he is a Lhomwe so support home industry took precedence,and secondly,by the time of appointing Cabinet Mins,he was around and close. Such being the case,he got the job. Now he said those careless words to please his master Peter. Madam Banda! U must settle this in… Read more »
mumanena thinking kuti sabwera eti.
See now akubweratu mwayamba be out- of- court-settlement.
Ayinso be inside court-settlement.
Anthu ambiri amene mumaika ma comment apa mukuwoneka kuti ndinu ana. Kapena I should blame myself for being in the company of ana. Nankhumwa amaziyamba dala nkhanizi chifukwa he doesn’t want to sue himself koma kuti okhudzidwayo akasume for defamation kenako akatulutse ma backup evidence pa court. ngati mumakhaladi pa Malawi pompano munditsimikiza kuti palibe move imene DPP inalepherako. Ngakhale ma CCTV footage aja alipodi koma akungodikira zomuwawayo akasume chifukwa mulandu otero siuvuta.
Iwe, these people should not use you. See you have a long way to go and still fresh, open your eyes.
Kungokamba zinkhani kuti asangalatse abwana awo. I just wonder if Kondwani has brains.
Kufuna kuonetsa ngati President wathu ndi mchabwa. Msiyeni Mutharika naye mavuto ngosayamba.
Please learn to tame your tongue Mr Minister. You are not an object but a human like everyone else.