Email a copy of 'DePeCo invades Kasungu with message of hope, thousands of people attend rally' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

7 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
John
John
6 years ago

Koma wosakomo zimene mukuwonazo sizinayambe zenizeni muziwona tizipani tizipani tanu tosawukato kudalira ndalama zamunthu monzi mulira Chaka chake ndichino MCP nkachaniso.

Jajah
Jajah
6 years ago

The mighty party 2019 Dr.Chris Daza Boma viva DEPECO viva Dr Chris Daza viva wina alira akuwona ngati anthu akusapota zipani chifukwa cha agogo awo pano anthu anazindikira MCP ndi DPP sizipaniso za agogo DEPECO chachinyamata sitikufunaso nkhalamba.

kaka ni dada
kaka ni dada
6 years ago

Bambo Daza kodi mwayimitsako ma councillors ku Milonde ndi ku Malindi kapena ka chipani kanu kakadali mu chikwama , mukamati democratic people’s congress mwati basi kachipani kameneka kalowa mmalo mwa MCP, zosatheka muwafunse a Nthanda Congress party (NCP) kuti anathela kuti akuwuzani. Ife takonzeka kutulutsa DPP m’boma ndi Chakwera. Anthu enanu dyera, munathawa ku MCP chifukwa sanakusankheni pa upulezidenti wa chipani ku convention. Muzingolubwalubwa choncho basi!

Mbuyache
Mbuyache
6 years ago

It makes some people feel happy when they see a group of people in front of them showering praises………so keep on dreaming sir and enjoy life.

MAGUFULI
MAGUFULI
6 years ago

MALAWI NEEDS REVOLUTION !

MALAWI NEEDS EVANGALISATION !

MALAWI NEEDS COMPLETE OVERHAUL

MALAWI NEEDS NEW LEADERS

MALAWI NEEDS YOUNG VIBRANT
LEADERS

BUSHIRI IS THE MAN OF OUR
GENERATION !!

kaka ni dada
kaka ni dada
6 years ago

ADaza akudyerani anyamata ndi atsikana a mu KU

chajunda wa ku ntcheu
6 years ago
Reply to  kaka ni dada

Yayi ku kasungu ni kwa tambara wa kuda imwe namwe.Akungo kugwirani mmaso chaje.

Read previous post:
Malawi police arrest Northern Region immigration chief

Malawi police from Area 30 headquarters in Lilongwe have arrested the northern region immigration chief over immigrants syndicate. Police are...

Close