Email a copy of 'DPP counters MCP: ‘Kamuzu was also hiring planes, picking hangers on’' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'DPP counters MCP: ‘Kamuzu was also hiring planes, picking hangers on’' to a friend
World Bank has tipped Malawi and other sub-Saharan Africa countries who are continuing to grow, albeit at a slower pace,...
wabwino ndi Yesu basi forever the rest are nothing even Obama u cant compare
chonde,a dpp pofuna kudziteteza muziyamba mwakonzeka kaye,mwaonetsa kuti zonyasa mukuchita dala poti kale zidachitikapo kuganizila konyasa ndipo mukuyankha poti inu simukuvutika koma omwe adavota kukanakhala kuti munawapatsa zizindikiro bola adzakuvotelaninso apo ayi mayankho amene mudzankhila muli kwa chimaliro.sibwino kuyankha mokhumudwitsa anthu kuti abwezele kupusa konse kukhoza kuthela pompo
Yes! Kamuzu was hiring planes but it was worth it. Malawi kwacha was equal to a pound. Simungayerekeze zinyatsi za president za masiku anozi.Bwanji chipongwe kodi? Kodi ku Malawi tili ndi president pano?
muno mumalawit president alipo.nanga mukumukwenya za ndege ndindani.
Vito la mvp neologism kwao ndikususa basic. Kaya chabwino„chachabe iwo nyimbo Yawona ndikusutsa basi chifukwa anakhwima ndi kusutsa. Azakhala osutsa mpaka yeah azabwela
Komadi zinazi ndi mbuzidi. Sizowona kuti poti Kamuzu sianadzudzulidwe atachita kanthu ndiye kuti kukudzudzulani pano nkulakwa ayi. Mwina oganiza chinchiwa anali ana mnthawi ya ANGWAZI. Sizimatheka kudzudzulako. Mnthawi ino chitani zija mumkatuzuka nazo kulonjeza nthawi ya kampeni ija. TIKUKUONANITU.
that was b4 multipaty. komanso by then chuma chimayenda bwino
resistance to change. Mind you this is onether century. You will die rich koma anthu opanda mtendere. Zitsilu ndi ovotafe sitiona kutali amalawi kugona warm heart of zitsilu.
R u doing it bcoz Kamuzu (or MCP) was doing it. With this kind of thinking, can we expect any meaningful change from these idiots? Kamuzu amachita zimenezi akubalansa mabuku, ndalama zamadona zikubwera, etc. Dikirani mastraka ayambe. Enanu simuthawa? Ndiposo ulendo uno ophedwa achuluka. Malo moti muzikhala phe, mwalakwa nkumachulukaso zonena. Sikukala pabala kumeku?
R u doing it bcoz Kamuzu (or MCP) was doing it. With this kind of thinking, can we expect any meaningful change from these idiots? Kamuzu amachita zimenezi akubalansa mabuku, ndalama zamadona zikubwera, etc. Dikirani mastraka ayambe. Enanu simuthawa. Ndiposo ulendo uno ophedwa achuluka. Malo moti muzikhala phe, mwalakwa nkumachulukaso zonena. Sikukala pabala kumeku.
@Olomwe, Alomwe onse akanakhala ngati iwe mwenzi dziko lino ndilotuka so kpon educating ur fellow Lomwez to know the truth.