Email a copy of 'DPP counters MCP: ‘Kamuzu was also hiring planes, picking hangers on’' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

190 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
Davis Zikonyani
8 years ago

wabwino ndi Yesu basi forever the rest are nothing even Obama u cant compare

hannock chituvi
8 years ago

chonde,a dpp pofuna kudziteteza muziyamba mwakonzeka kaye,mwaonetsa kuti zonyasa mukuchita dala poti kale zidachitikapo kuganizila konyasa ndipo mukuyankha poti inu simukuvutika koma omwe adavota kukanakhala kuti munawapatsa zizindikiro bola adzakuvotelaninso apo ayi mayankho amene mudzankhila muli kwa chimaliro.sibwino kuyankha mokhumudwitsa anthu kuti abwezele kupusa konse kukhoza kuthela pompo

Nankununkha sadzimva
Nankununkha sadzimva
8 years ago

Yes! Kamuzu was hiring planes but it was worth it. Malawi kwacha was equal to a pound. Simungayerekeze zinyatsi za president za masiku anozi.Bwanji chipongwe kodi? Kodi ku Malawi tili ndi president pano?

mr diamond
mr diamond
8 years ago

muno mumalawit president alipo.nanga mukumukwenya za ndege ndindani.

musisipala
8 years ago

Vito la mvp neologism kwao ndikususa basic. Kaya chabwino„chachabe iwo nyimbo Yawona ndikusutsa basi chifukwa anakhwima ndi kusutsa. Azakhala osutsa mpaka yeah azabwela

ndondochandata
8 years ago

Komadi zinazi ndi mbuzidi. Sizowona kuti poti Kamuzu sianadzudzulidwe atachita kanthu ndiye kuti kukudzudzulani pano nkulakwa ayi. Mwina oganiza chinchiwa anali ana mnthawi ya ANGWAZI. Sizimatheka kudzudzulako. Mnthawi ino chitani zija mumkatuzuka nazo kulonjeza nthawi ya kampeni ija. TIKUKUONANITU.

stephen
stephen
8 years ago

that was b4 multipaty. komanso by then chuma chimayenda bwino

chalaza
chalaza
8 years ago

resistance to change. Mind you this is onether century. You will die rich koma anthu opanda mtendere. Zitsilu ndi ovotafe sitiona kutali amalawi kugona warm heart of zitsilu.

Malawi wa Lero
Malawi wa Lero
8 years ago

R u doing it bcoz Kamuzu (or MCP) was doing it. With this kind of thinking, can we expect any meaningful change from these idiots? Kamuzu amachita zimenezi akubalansa mabuku, ndalama zamadona zikubwera, etc. Dikirani mastraka ayambe. Enanu simuthawa? Ndiposo ulendo uno ophedwa achuluka. Malo moti muzikhala phe, mwalakwa nkumachulukaso zonena. Sikukala pabala kumeku?

Malawi wa Lero
Malawi wa Lero
8 years ago

R u doing it bcoz Kamuzu (or MCP) was doing it. With this kind of thinking, can we expect any meaningful change from these idiots? Kamuzu amachita zimenezi akubalansa mabuku, ndalama zamadona zikubwera, etc. Dikirani mastraka ayambe. Enanu simuthawa. Ndiposo ulendo uno ophedwa achuluka. Malo moti muzikhala phe, mwalakwa nkumachulukaso zonena. Sikukala pabala kumeku.

Denguzman
8 years ago

@Olomwe, Alomwe onse akanakhala ngati iwe mwenzi dziko lino ndilotuka so kpon educating ur fellow Lomwez to know the truth.

Read previous post:
World Bank tips Malawi on economic growth: Caution on subsidies splurge

World Bank has tipped Malawi and other sub-Saharan Africa countries who are continuing to grow, albeit at a slower pace,...

Close