Email a copy of 'DPP courts Ndirande, Nankhumwa to hold ‘mega’ political rally' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

12 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
Akulu
Akulu
5 years ago

Funny tiyeni nazo pa ndix mukawauze zomwe mwawachitira

mtete
mtete
5 years ago

I wish Nankhumwa well and mynadvice is not to let idiot Mchacha spoil the show through his uncouth utterances. We will be listening. Yes, Ndirande was once a DPP no go area. Not any more. MCP and UTM have acquired several plots there.

Alamu Pumani Mwakula kuba

George Malemia anzako ngati Chaponda and Henry Mussa ali kuti? Mwanavekha and Fabiano samveka. Uladi bwanji osawagawira a Goodall Gondwe ndi a Msaka azikazi uli nawo aja. Nanga atatu wekha?

Ndatopa
Ndatopa
5 years ago

A dad atopa sakwanisa?

mediaz
mediaz
5 years ago

Nkhani ndiyokuti mwamusiyila nankhumwayi kapena?Isaa!! Tiuzeni zoona pano,,,,,,,DPP yagawikana some people follow this boy nankhumwa and the other camp supporting Ben Phiri….puludzu!!

Kalulu Wadwala
Kalulu Wadwala
5 years ago

Tsono ife a ku ndix mwadziwa lero kuti tikusowa clean water, there is high unemployment? Be serious with your cheap politics. Kwanu mwayika miseu ya phula kumalo kuti ndikumidzi palibe chingathandize malo moganizira ife a ndirande? Bwerani muzaname monga mumachitichira nthawi zonse. Tizaonana May 2019

Kalulu 2018
5 years ago

Kodi campaign mukusiira nankhumwa bwanji? Kapena ticket nja nankhumwa-atupele?? Kapena nankhumwa- joyce banda’s son? Koma amalawi anthu atipezelera ngati akwa nyezelera!

Paramount Chief wa ku Thyolo
Paramount Chief wa ku Thyolo
5 years ago

Anyapapi nyapapilizing fellow nyanyipers zapa ndix….mukachoka apo mukakwatane…..mulibe nseru?

James
5 years ago

Mulibe ulesi,azikamvera mbavayo ndiye ndani? Mukufuna kudzatinamiza Kuti chiyani? Bwerani mudzatipeza muzayiziwa Ndix..

Napoleon Muza
5 years ago
Reply to  James

James, do vetting of all those that are on the fore front of Chilima and tell me they are clean. Do vetting on Masangwi , Kaliati, Lucius, . Have you even forgotten that mang’anya is a rapist. Do vetting and then open your dirty mouth. Msowoya , tractorgate etc.

Mulupale
Mulupale
5 years ago
Reply to  Napoleon Muza

You have still not exonerated the alleged thieves in James’s post. You have just mentioned more thieves I guess.

Dipipi wa Yudiefu
Dipipi wa Yudiefu
5 years ago
Reply to  Napoleon Muza

What you are talking about are allegation, issues that have not proved in a court of law. How do you explain the other side? The one going to talk on behalf of DPP has a stolen certificate. His bosses have decided to anchor the back bench because they have discovered that they can not lie forever. 145 million thief, maize thief, education money thief, immigration money thief, Esom money thief. So, the certificate man is better than the big thieves. A better strategy I suppose.

Read previous post:
UTM victory has started, says Chilima: Malawi veep vows to defend democracy ‘relentlessly’

Vice President Saulos Chilima has said Friday’s court ruling to register UTM as a political party is the start of...

Close